24
CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU 1. Ndikhulupirira Mulungu Atate, Wamphamvuyonse, Wolenga zakumwamba ndi zapansi; 2. Ndikhulupirira Yesu Khristu, Mwana wake wobadwa yekha, Ambuye wathu; 3. Amene anapatsidwa ndi Mzimu Woyera, nabadwa mwa Mariya namwaliyo; 4. Nasautsidwa kwa Pontio Pilato; napachikidwa pamtanda, nafa, naikidwa m’manda, natsikira kwa akufa; 5. Tsiku lachitatu anaukanso kwa akufa; 6. Nakwera kumwamba, nakhala padzanja lamanja la Mulungu Atate Wamphamvuyonse; 7. Kudzera komweko adzadza kudzaweruza anthu amoyo ndi akufa; 8. Ndikhulupirira Mzimu Woyera; 9. Ndkhulupirira Mpingo Wopatulika wa Khristu, wa kwa anthu onse, chiyanjano cha oyera mtima mtima; 10. Kukhululukidwa kwa machimo; 11. Kuukanso kwa thupi; 12. Ndi moyo wosatha. AMEN. MALAMULO KHUMI 1. Usakhale nayo milungu yina koma Ine ndekha. 2. Usadzipangire iwe wekha fano losema, kapena chifaniziro chirichonse cha zinthu za m’thambo la kumwamba kapena kapena za m’dziko lapansi, kapena za m’madzi a pansi pa dziko. 3. Usatchule dzina la Yehova Mulungu wako pachabe. 4. Udzikumbukira tsiku la Sabata, likhale lopatulika. 5. Uzilemekeza atate wako ndi amako, kuti achuluke masiku ako m’dziko limene Yehova Mulungu wako akupatsa iwe. 6. Usaphe. 7. Usachite Chigololo. 8. Usabe. 9. Usamnamizire mnzako. 10. Usasirire. PEMPHERO LA AMBUYE Atate wathu wakumwamba: Dzina Lanu liyeretsedwe; Ufumu Wanu udze; Kufuna kwanu kuchitidwe; Monga kumwamba; Chomwecho pansi pano. Mutipatse ife lero; Chakudya chathu chalero. Ndipo mutikhululukire zochimwa zathu; Monga ifenso tiwakhululukira amangawa athu. Musatitengere ife kokatiyetsa; Koma mutipulumutse ife kwa oipayo. Chifukwa wanu ndi Ufumu, ndi Mphamvu, ndi Ulemerero wa nthawi zonse. AMEN. 1

CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

  • Upload
    others

  • View
    3

  • Download
    0

Embed Size (px)

Citation preview

Page 1: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU1. Ndikhulupirira Mulungu Atate,

Wamphamvuyonse, Wolengazakumwamba ndi zapansi;

2. Ndikhulupirira Yesu Khristu, Mwanawake wobadwa yekha, Ambuyewathu;

3. Amene anapatsidwa ndi MzimuWoyera, nabadwa mwa Mariyanamwaliyo;

4. Nasautsidwa kwa Pontio Pilato;napachikidwa pamtanda, nafa,naikidwa m’manda, natsikira kwaakufa;

5. Tsiku lachitatu anaukanso kwa akufa;6. Nakwera kumwamba, nakhala

padzanja lamanja la Mulungu AtateWamphamvuyonse;

7. Kudzera komweko adzadzakudzaweruza anthu amoyo ndi akufa;

8. Ndikhulupirira Mzimu Woyera;9. Ndkhulupirira Mpingo Wopatulika wa

Khristu, wa kwa anthu onse,chiyanjano cha oyera mtima mtima;

10. Kukhululukidwa kwa machimo;11. Kuukanso kwa thupi;12. Ndi moyo wosatha. AMEN.

MALAMULO KHUMI1. Usakhale nayo milungu yina koma Ine

ndekha.2. Usadzipangire iwe wekha fano losema,

kapena chifaniziro chirichonse chazinthu za m’thambo la kumwambakapena kapena za m’dziko lapansi,kapena za m’madzi a pansi pa dziko.

3. Usatchule dzina la Yehova Mulunguwako pachabe.

4. Udzikumbukira tsiku la Sabata, likhalelopatulika.

5. Uzilemekeza atate wako ndi amako,kuti achuluke masiku ako m’dzikolimene Yehova Mulungu wakoakupatsa iwe.

6. Usaphe.7. Usachite Chigololo.8. Usabe.9. Usamnamizire mnzako.

10. Usasirire.

PEMPHERO LA AMBUYEAtate wathu wakumwamba:Dzina Lanu liyeretsedwe;Ufumu Wanu udze;Kufuna kwanu kuchitidwe;Monga kumwamba;Chomwecho pansi pano.Mutipatse ife lero;Chakudya chathu chalero.Ndipo mutikhululukire zochimwa zathu;Monga ifenso tiwakhululukira amangawa athu.Musatitengere ife kokatiyetsa;Koma mutipulumutse ife kwa oipayo.Chifukwa wanu ndi Ufumu, ndi Mphamvu, ndi Ulemerero wa nthawi zonse. AMEN.

1

www.princexml.com
Prince - Non-commercial License
This document was created with Prince, a great way of getting web content onto paper.
Page 2: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

MAU OYAMBILIRAAbale ndi alongo mwa Ambuye. Katikisimu ndi buku mmene malangizo ake kapenachiphunzitso chake chimakhala ndi funso komanso yankho. Buku ili likutchedwaKatekisimu Wachidule kuti asiyanitsidwe ndi wina wankulu amene mafunsowaatanthauziridwa kwambiri. Katekisimuyi analembedwa mchaka cha 1647 ndi abusaosiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwaWestminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande.Abusawatu amakonza madziko a mpingo wamoyo wa Ufumu Wa Mulungu.Katekisimu ali ndi mafunso komanso mayankho okwana 107. Mafunso oyambiliraatatu ndi ongotitsogolera. Kenako pali mafunso 33 (kuchokera funso 4 mpaka 38).Mafunso 33 amenewa amatiuza zimene ife tiyenera kukhulupirira. Mafunso ena onseotsalawo omwe ndi 69 (funso 39 mpaka 107) amatiuza zimene ife tiyenera kumachita.

Bukuli ndi lofunika kwambiri kwa Mkhristu aliyense chifukwa mafunso onse 107amangika pa madziko a Chikhristu. M’buku ili mafunsowa agawidwa m’magawoaafupi kuti munthu wowerenga ndi wophunzira bukuli athe kutsatira bwino.

Mubulinso muli mavesi a m’Baibulo amene akuperekera umboni wa funso liri lonsendipo kutsimikizira kuti mayankho onsewa achokera mu Buku limeneli lomwe ndiLopatulika chifukwa ndi Mau A Mulungu.

Kumapeto a bukuli taikanso mafunso onse 107 ngati kubwereza kuti owerengaaonesetse kuti akutsatiradi ndipo ngati nkotheka kuloweza mafunso ndi mayankhoonse. Kumayambiliro monga mmene mwaonera mulinso Chikhulupiriro cha Akhristu,Malamulo Khumi, komanso Pemphero La Ambuye zimene Akhristu a EvangelicalPresbyterian Church ayenera kuloweza pamtima.

Ambuye akudalitseni nonse pamene muli pa ntchito yotamandika ngati imeneyiyowerenga ndi kuloweza Katikisimuyi kuti moyo wanu wa uzimu upite patsogolozimenenso zipangitse kuti mpingo wathu upite patsogolo.

Rev. Rex ChitekweRev. Rex ChitekweM’malo mwa Evangelical Presbyterian Church Synod Executive CommitteeM’malo mwa Evangelical Presbyterian Church Synod Executive CommitteeMay, 2012

2

Page 3: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

KATEKISIMU WACHIDULE WA WESTMINSTERFUNSOFUNSO 1.1. KodiKodi cholingacholinga chenichenichenichenichimenechimene munthumunthu ayeneraayenera kuchitakuchita kwakwaMulungu ndi chiyani?Mulungu ndi chiyani?YANKHO. Cholinga chenicheni chimenemunthu ayenera kuchita ndikokulemekeza Mulungu ndi kukondwereramwa Iye nthawi zonse.1 Akorinto 10:31; “chifukwa chake mungakhalemudya, mungakhale mumwa, mungakhale muchitakanthu kena, chitani zonse ku ulemerero waMulungu”. Masalimo 73:25-26; “Ndiri ndi yanikumwamba koma Inu? Ndidpo padziko lapansipalibe wina wondikonda koma Inu. Likatha thupilanga ndi mtima wanga: Mulungu ndiye thanthwe lamtima wanga, ndi chodalira change chosatha”.

FUNSOFUNSO 2.2. KodiKodi ndindi lamulolamulo litiliti lomwelomweMulunguMulungu waperekawapereka lotitsogoleralotitsogolera ifeifem’menetingamlemekezerem’menetingamlemekezere ndindikukondwerera mwakukondwerera mwa Iye?Iye?YANKHO. Mawu a Mulungu amene alim’Chipangano Chakale ndi Chatsopanondi okhawo amene ali lamulo lotitsogoleraife m’mene tingamlemekezere ndikukondwera mwa Iye.Aefeso 2:20; “Omangika padziko atumwi ndianeneri pali Khristu Yesu mwini, mwala wapangodya”. 2 Petro 3:7; “Koma miyamba ndi dzikola masiku ano, ndi mawu omwewo zaikika kumoto,zasungika kufikira tsiku la chiweruzo ndichiwonongeko cha anthu osapembedza”. 2 Timothy3:16; “Lemba lililonse adaliuzira Mulungu, ndipolipindulitsa pa chiphunzitso, chitsutsano,chikonzero,chilangizo cha nchilungamo”’.

FUNSOFUNSO 3.3. KodiKodi mawumawu aa MulunguMulungukwenikweni amaphunzitsa chiyani?kwenikweni amaphunzitsa chiyani?YANKHO. Mawu a Mulungu kwenikweniamphunzitsa chimene munthu ayenerakukhulupirira chokhuza Mulungu, ndiudindo wa munthu kwa Mulungu.2 Timoteo 1:13; “Gwira chitsanzo cha mawu amoyo, amene udawamva kwa ine, mwachikhulupiliro ndi chikondi chili mwa Khristu Yesu”.

GAWO LOYAMBA :ZIMENE TIYENERAKUKHULUPIRIRA1. M’MENE MULUNGU ALILIFUNSO 4.FUNSO 4. Kodi Mulungu ndi ndani?Kodi Mulungu ndi ndani?YANKHO. Mulungu ndi Mzimu, Wopandamalire, wamuyaya ndi wosasinthika, mukukhala kwake, mu nzeru, mu mphamvu,mu chiyero, mu chilungamo, mu ubwinondipo muchoonadi chake.Yohane 4:24; “Mulungu ndiye Mzimu, ndipoomulambira Iiye amulambire mu Mzimu ndimchoonadi”. Yobu 11:7 “Kodi ukhoza kupezaMulungu mwa kufunafuna? Ukhoza kupezawamphamvu yonse motsindika”? Masalimo 90:2;“Asanabadwe mapiri, kapena musanalenge dzikolapansi, ndi lokhalamo anthu, Inde, kuyambiranthawi yosayamba kufikira nthawi yosatha, Inundinu Mulungu”.

FUNSO 5.FUNSO 5. Kodi ilipo Milungu inanso?Kodi ilipo Milungu inanso?YANKHO. Pali Mulungu m’modzi yekha,wa moyo ndi woona.Deutronomo 6:4; “Imvani, Israeli Yehova Mulunguwathu, Yehova ndiye m’modzi”. Yeremiya 10:10;“Koma Yehova ndiye Mulungu woona, ndiyeMulungu wamoyo, Mfumu yamuyaya; pa mkwiyowake wa dziko lapansi lidzanthunthumira ndiamitundu sangapilire ukali wake”.

FUNSOFUNSO 6.6. KodiKodi mumu UmulunguUmulungu mulimuli anthuanthuangati?angati?YANKHO. Mu Umulungu muli anthu atatu:Atate, Mwana ndi Mzimu Woyera. Ndipoatatuwa ali Mulungu m’modzi, ofananamuchikhalidwe, mu mphamvu ndi muulemerero.Mateyu 28:19; “Chifukwa chake mukaniphunzitsani anthu amitundu yonse ndi kuwabatizaiwo m’dzina la Atate, ndi la Mwana ndi la MzimuWoyera”. 1 Yohane 5:7; “Ndipo Mzimu ndiyewakuchita umboni chifukwa Mzimu ndiyechoonadi”.

3

Page 4: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

2. ZIMENE MULUNGU WACHITAFUNSOFUNSO 7.7. KodiKodi malamulomalamulo aa MulunguMulungu ndindiotani?otani?YANKHO. Zolinga za Mulungu zili zosathamolingana ndi uphungu wa chifunirochake kotero kutimwaulemerero wake Iyeanakonzeratu zinthu zinse zochitika.Aefeso 1:11-12; “Mwa Iye tinayesedwa cholowachake, popeza tinakonzekeratu monga mwachitsimikizo mtima chake Iye wakuchita zonsemonga uphungu wa chifuniro chake; kuti ifetikayamikitse ulemerero wake”.

FUNSOFUNSO 8.8. NangaNanga MulunguMulungu akukwaniritsaakukwaniritsabwanji malamulobwanji malamulo ake?ake?YANKHO. Mulungu akukwaniritsamalamulo ake muntchito zachilengedwendi muchisamaliro.Chibvumbulutso 4:11; “Muyenera Inu Ambuyewathu, ndi Mulungu wathu, Kulandira ulemererondi ulemu ndi mphamvu; chifukwa mudalengazonse, ndipo mwa chifuniro chanu zinakhala Ndipozinalengedwa”. Danieli 4:35; “Ndi okhala padzikoonse ayesedwa achabe, ndipo Iye achita mwachifuniro chake m’khamu lakumwamba ndi mwaokhala pa dziko lapansi; ndipo palibe woletsadzanja lake, kapena wakunena naye muchitanji”?

3. CHILENGEDWEFUNSOFUNSO 9.9. KodiKodi ntchitontchito yaya chilengedwechilengedwendi yotani?ndi yotani?YANKHO. Ntchito ya chilengedwe ndikokupangidwa kwa zinthu zonse ndiMulungu kuchokerapopanda kanthu, mumphamvu ya mawu ake m’masiku asanundi limodzi ndipo zonse zinali bwino.Genesis 1:1; “Pachiyambi Mulungu analengakumwamba ndi dziko lapansi”. Ahebri 11:3; “Ndichikhulupiriro tizindikira kuti maiko onse, ndi am’’mwamba omwe anakonzedwa ndi mawu aMulungu, kotero kuti zinthu zopenyekasizinapangidwa zochokera mwa zoonekazo”.Genesis 1:31; “Ndipo adaziwona Mulungu zonsezimene adazipanga ndipo taonani, zinali zabwinondithu. Ndipo panali madzulo ndipo panalim’mawa, tsiku lachisanu ndi chimodzi”.

FUNSOFUNSO 10.10. KodiKodi munthumunthu analengedwaanalengedwabwanji?bwanji?YANKHO. Mulungu analenga munthu,mwamuna ndi mkazi mu chifanizirochake, muchidziwitso, m’chilungamo ndim’chiyero ndikuti alamulire pazolengedwazonse.Genesis 1:27; “Mulungu ndipo adalenga munthumuchifanizo chake, muchifanizo cha Mulunguadamulenga iye; adalenga iwo mwamuna ndimkazi”. Genesis 1:28; “Mulungu ndipo anadalitsaiwo, ndipo adati kwa iwo, mubalane muchuluke,mudzadze dziko lapansi, muligonjetse; mulamulirepa nsomba za mnyanja ndi mbalame zamlengalenga ndi pa zonse za moyo zakukwawa padziko lapansi”.

4. NTCHITO ZA MULUNGU MUCHISAMALIRO CHAKEFUNSOFUNSO 11.11. KodiKodi ntchitontchito zaza MulunguMulungumuchisamaliro chake ndi zotani?muchisamaliro chake ndi zotani?YANKHO. Ntchito za Mulungu

muchisamaliro chake ndi chiyero chake,nzeru zake ndi mphamvuyakusunga ndikulamulira zolengedwa zake ndizichitochito zawo.Masalimo 145:17; “Yehova ali wolungama m’njirazake zonse. Ndi wachifundo m’ntchito zakezonse”. Yesaya 28:29; “Ichinso chifumira kwaYehova wa makamu, uphungu wake uzizwitsa ndinzeru yake ipambana”.

FUNSOFUNSO 12.12. KodiKodi ndindi chisamalirochisamalirochapaderachapadera chotanichotani chimenechimene MulunguMulunguanaonetseraanaonetsera kwakwa munthumunthu m’mundam’mundaumene analengedwera?umene analengedwera?YANKHO. Pamene Mulungu analengamunthu, munthuyo analowa muchipangano cha moyo ndi iyepakulonjeza. kumvera kwa ngwiro;kumuletsa iye kudya chipatso chamtengowodziwitsa zabwino ndi zoipaumene unali ndi ululu wa imfa.Agalatiya 3:12, “ Koma chilamulo sichichokera kuchikhulupiliro; koma wakuzichita izi adzakhala ndimoyo ndi izi”. Genesis 2:17, “koma mtengo

4

Page 5: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

wakudziwitsa zabwino ndi zoipa usadye, chifukwatsiku limene udzadye udzafa ndithu” .

5. MMENE MUNTHU ANACHIMWIRAFUNSOFUNSO 13.13. KodiKodi makolomakolo anthuanthu oyambaoyambaanapitiliraanapitilira kukhalabekukhalabe m’menem’meneadalengedwera?adalengedwera?YANKHO. Makolo athu oyambapopatsidwa ufulu wa chifuniro cha iwoeni, anagwa ndi kuchokammeneanalengelengedwera ndi Mulungu.Deutronomo 30:19; “Ndichititsa mboni lerokumwamba ndi dziko lapansi zitsutse inu; ndaikapakati panu moyo ndi imfa, mdalitso ndi temberero;potero sankhani moyo kuti mukhale ndi moyo, inundi mbeu zanu”. Mlaliki 7: 29, “Taonani ichichokha ndachipeza kuti Mulungu analenga anthuoongoka mtima; koma iwowa anafunafunamalongoseledwe a mitundu mitundu”.

FUNSO 14.FUNSO 14. Kodi tchimo ndi chiyani?Kodi tchimo ndi chiyani?YANKHO. Tchimo ndi kulephera kuchitachifuniro cha Mulungu kapenakuphwanya malamulo aMulungu.Luka 10: 31; “Ndipo kudangotero kuti wansembewina anatsika njirayo, ndipo pakumuona iye anapitambali yina”. Luka 22:61; “Ndipo Ambuyeanapotoloka, nayang’ana Petro. Ndipo Petroakumbukila mau a Ambuye, kuti anati kwa iye,asanalire tambala lero lino, udzandikana Inekatatu”.

FUNSOFUNSO 15.15. KodiKodi ndindi tchimotchimo lanjilanji limenelimenelinapangitsalinapangitsa makolomakolo athuathu oyambaoyamba kugwakugwakuchokera m’manja mwa Mulungu?kuchokera m’manja mwa Mulungu?YANKHO. Tchimo limene linapangitsamakolo athu oyamba kugwa kuchokeram’manja mwaMulungu ndilo kudyachipatso choletsedwa.Genesis 3: 6-8; “Ndipo pamene anaona mkaziyokuti mtengo unali wabwino kudya, ndi kuti unaliwokoma m’maso, mtengo wolakalakika wakupatsanzeru, anatenga zipatso zake, nadya, napatsansomwamuna wake amene anali naye, nadya iyenso”.

6. ZOTSATIRA ZAKUCHIMWA KWAMUNTHUFUNSOFUNSO 16.16. KodiKodi mtundumtundu wonsewonse wawa anthuanthuunachimwansounachimwanso pamenepamene AdamuAdamuanachimwakoyamba?anachimwakoyamba?YANKHO. Pokhala chipanganochinachitika pakati pa Mulungu ndiAdamu, osati kwa iye yekhakomanso ndimbewu yake, mtundu wa anthu onseochokera mwa iye monga mwamibadwo,anachimwa naye limodzi mu tchimo lakeloyamba.Aroma 5: 18, 19; “Chifukwa chake, monga mwakulakwa kumodzi kutsutsa kunafikira anthu onse;chomwechonso . Pakuti monga ndikusamvera kwamunthu mmodzi ambiri anayesedwa ochimwa”. 1Akorinto 15: 22; “Pakuti monga mwa Adamu onseamwalira, choteronso mwa Khristu onseakhalitsidwa ndi moyo”.

FUNSOFUNSO 17.17. NangaNanga kugwakugwa kwakwa AdamuAdamukunabweretsakunabweretsa chiyanichiyani kuku mtundumtundu wawaanthu?anthu?YANKHO. Kugwa kwa Adamukunabweretsa tchimo ndi mazunzo kumtundu wa anthu.Aroma 5:12; “Chifukwa chake monga uchimounalowa m’dziko mwa munthu m’modzi ndi imfamwa uchimo; kotero imfa inafikira anthu onse,chifukwa kuti onse anachimwa”.

FUNSOFUNSO 18.18. KodiKodi tchimotchimo limenelimene linafikiralinafikiramunthu limapezeka mu chiyani?munthu limapezeka mu chiyani?YANKHO. Uchimo umenewu unapezekamu tchimo la Adamu, mukuperewera kwachilungamochapachiyambi, komansokuonongeka kwa chikhalidwe chakechonse, kumene kumatchedwa tchimolapachiyambi, pamodzi ndi zonsezotuluka mmenemo.Aroma 5:19; ‘’Pakuti monga ndi kusamvera kwamunthu m’modzi ambiri anayesedwa ochimwa”.Masalimo 51:5; “Onani ndinabadwa mphulupulundipo amayi wanga anandilandira m’zoipa”.

5

Page 6: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

FUNSOFUNSO 19.19. KodiKodi ndindi masautsomasautso otaniotaniameneamene anabweraanabwera kwakwa munthumunthu chifukwachifukwacha uchimo?cha uchimo?YANKHO. Mtundu wonse wa anthuunataya chiyanjano ndi Mulungu chifukwacha uchimo ndipo iwo uli pansi pa mkwiyondi temberero lake ndi kuwabweretseramasautso a moyo uno, a imfa, ndizowawa za ku gahena kunthawi zosatha.Yesaya 59:2; “Koma zoipa zanu zakulekanitsani inundi Mulungu wanu; ndipo machimo anu abisankhope yake kwa inu, kuti Iye sakumva. Ezekiel18:4; “Moyo wochimwawo ndiwo udzafa”.

7. CHIPULUMUTSOFUNSOFUNSO 20.20. KodiKodi MulunguMulungu analekeleraanalekeleramtundumtundu wawa anthuanthu kutikuti uwonongekeuwonongekem’machimo ndi m’masautsom’machimo ndi m’masautso awo?awo?YANKHO. Popeza chifuniro cha Mulungundi chabwino, anasankha ena ku moyowosatha kulowa nawo mu Pangano laChisomo, pa kuwavuula mu uchimo ndim’mavuto ndi kuwayika iwom’chiwombolo chochitidwa ndiMPULUMUTSI.Genesis 3:15; “Ndipo ndidzaika udani pakati pa iwendi mkaziyo, ndi pakati pa mbeu yako ndi mbeuyake; ndipo idzalalira mutu wako, ndipo iweudzalalira chitende chake. 2 Timoteo 1:9; “ Ameneanatipulumutsa ife, natiitana ndi maitanidwe oyera,simonga ndi ntchito zathu, komatu monga mwachitsimikizo mtima cha Iye yekha, ndi chisomo,chopatsika kwa ife mwa Khristu Yesu zisanayambenthawi zoyamba”.

FUNSOFUNSO 21.21. KodiKodi MpulumutsiMpulumutsi wawa anthuanthuosankhidwa a Mulungu ndi ndani?osankhidwa a Mulungu ndi ndani?YANKHO. Mpulumutsi wa osankhidwa aMulungu ndi Ambuye Yesu Khristu,amene pokhalaMwana wa Mulungu,ANASANDUKA MUNTHU, ndipoanakhalabe , ndipo akupitirizakukhala,MULUNGU NDI MUNTHU, kwa muyaya.Machitidwe 4:12; “Ndipo palibe chipulumutso mwawina aliyense, pakuti palibe dzina lina pansi pathambo la kumwamba, lopatsidwa mwa anthu,limene tiyenera kupulumutsidwa nalo”. Ahebri 2:

14; “Popeza tsono ana ndiwo a mwazi ndi nyama,Iyenso momwemo adalawa nao makhalidweomwewo kuti mwa imfa akamuononge iye ameneanali nayo mphamvu ya imfa, ndiye mdierekezi”.

FUNSOFUNSO 22.22. KodiKodi KhristuKhristu pokhalapokhala mwanamwanawa Mulungu anakhala bwanji munthu?wa Mulungu anakhala bwanji munthu?YANKHO. Khristu Mwana wa Mulunguanakhala munthu pakudzitengera kwa IyeYekha THUPILENILENI, NDI MOYO ndikubadwa mwa namwali Mariya kupyoleramu mphamvu ya Mzimu ndipo anabadwaopanda tchimo.Luka 1:35; “Ndipo mngelo anayankha, nati kwa iye,Mzimu Woyera adzafika pa iwe, ndi mphamvu yawamkulukulu idzakuphimba iwe: chifukwachakenso Choyeracho chikadzabadwa,chidzachedwa Mwana wa Mulungu”. Agalatiya 4:4;“Koma pokwaniridwa nthawi, Mulungu anatumaMwana wake wobadwa ndi mkazi, wobadwawakumvera lamulo”.

8. NTCHITO YA YESU MUCHIPULUMUTSOFUNSOFUNSO 23.23. KodiKodi ndindi maudindomaudindo atiati ameneameneKhristu ali nawo monga mombolo wathu?Khristu ali nawo monga mombolo wathu?YANKHO. Khristu monga mombolowathu akugwira ntchito yake mongaMNENERI, WANSEMBE komansoMFUMU, muchikhalidwe chakeCHODZICHEPETSA komanso muULEMELERO.Machitidwe 3: 22; “Mosetu anati, Mbuye Mulunguadzaukitsira inu mneneri mwa abale anu, ngati ine;mudzamvera iye m’zinthu ziri zonse akalankhulenanu.” Ahebri 5:6; “Monga anananso mwina, Iwendiwe wansembe wa nthawi zonse Monga mwadongosolo la Melikizedeke”.Masalimo 2:6 “Komaine ndadzoza mfumu yanga Pa Ziyoni, phiri langaloyera”.

FUNSOFUNSO 24.24. KodiKodi KhristuKhristu akugwiraakugwira bwanjibwanjintchito yake ya Uneneri?ntchito yake ya Uneneri?YANKHO. Khristu akugwira ntchito yakeya uneneri pakutiululira ife kupyolera mumau ake ndiMzimu Woyera muCHIFUNIRO CHAMULUNGU zokhuzachipulumutso Chathu.

6

Page 7: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

Yohane 16:13; Koma atadza Iyeyo, Mzimu wachoonadi, adzatsogolera inu m’choonadi chonse;pakuti sadzalankhula za Iye mwini; koma zinthuziri zonse adzazimva, adzazilankhula; ndipo zinthuzirinkudza adzakulalikirani”. Ahebri 1: 1, 2; “KaleMulungu analankhula ndi makolo mwa anenerim’manenedwe ambiri ndi mosiyana-siyana, komapakutha pake pa masiku ano analankhula ndi ifendi Mwana amene anamuika wolowa nyumba wazonse mwa Iyenso analenga maiko ndi am’mwamba omwe”.

FUNSOFUNSO 25.25. KodiKodi KhristuKhristu amagwiraamagwira bwanjibwanjintchito yake ya unsembe?ntchito yake ya unsembe?YANKHO. Khristu amagwira ntchito yakemonga wansembe pakuzipereka kwakeNSEMBE pokwaniritsa chilungamo cha uMulungu ndi kutiyanjanitsa ife ndiMulungu, komanso kutipembezera ife ifekosalekeza.Ahebri 4: 14; “Popeza tiri naye Mkulu wansembewamkuru, wopyoza miyamba, Yesu mwana waMulungu, tigwiritsitse chivomerezo chathu. Ahebri9:28; “Kotero Khristunso ataperekedwa nsembekamodzi kukasenza machimo a ambiri,adzaonekera pa nthawi yachiwiri, wopandauchimo, kwa iwo amene amlindirira, kufikirachipulumutso. Akolose 1:20; “Mwa Iyensokuyanjanitsa zinthu zonse kwa Iye mwini, atachitamtendere wa mtanda wake; mwa Iyetu, kapena zapadziko, kapena za m’mwamba”.

FUNSOFUNSO 26.26. NangaNanga KhristuKhristu anakwaniritsaanakwaniritsabwanji udindo wake monga mfumu?bwanji udindo wake monga mfumu?YANKHO. Khristu anakwaniritsa udindowake monga mfumu potikekera ife kwaIye yekha, pakulamulira ndi kutiteteza,kutigwiritsa ndi kugonjetsa adani athu ndiake.Masalimo 110:3 “Anthu anu adzadzipereka eni aketsiku la chamuna chunu: m’moyera mokometsetsa,mobadwira m’bandakucha, muli nao mame aubwana wanu.’ Yesaya 33: 22 “Pakuti Yehova ndiyewoweruza wathu, Yehova ndiye wotipatsamalamulo, Yehova ndiye Mfumu yathu ya Iyeadzatipulumutsa”. 1 Akorinto 15:25, “Pakutiayenera kuchita ufumu, kufikira ataika adani onsepansi pa mapazi ake”.

FUNSOFUNSO 27.27. KodiKodi kudzichepetsakudzichepetsa kwakwaKhristu kunali kotani?Khristu kunali kotani?YANKHO. Kudzichepetsa kwake kwaKhristu kunaonekera m’kubadwa kwakemnjira yodzichepetsa mwa lamulopodutsa mmavuto a moyo uno, mumkwiyo wa Mulungu ndi temberero la imfaya pamtanda, ndikuikidwa m’mandandikukhala pansi pa mphamvu ya imfakwakanthawi.Luka 2:7; “Ndipo Iye anabala mwana wake wamwamuna woyamba; namkulunga Iye m’salunam’goneka modyera ng’ombe, chifukwa kutianasowa malo mnyumba ya alendo”. Agalatiya 4:4;Koma pokwaniridwa nthawi Mulungu anatumaMwana wake wobadwa ndi mkazi, wobadwawakumvera lamulo” Yesaya 53:3; “Iyeananyozedwa ndikukanidwa ndi anthu, munthuwazisoni, ndi wodziwa zowawa; ndipoananyozedwa monga munthu wobisira anthunkhope zawo; ndipo ife sitinamulemekeza’.

FUNSOFUNSO 28.28. KodiKodi kupambanakupambana kwakwa YesuYesukunali kotani?kunali kotani?YANKHO. Kupambana kwa Yesu kunalipakuuka kwa akufa patsiku lachitatu ndikukweranso kumwamba, ndikukhalakudzanja la manja la Mulungu Atatendikubweranso kudzaweruza dziko lonselapansi pa tsiku lotsiriza.1 Akorinto 15:4; “Ndikuti anaikiidwa, ndikutianaukitsidwa tsiku lachitatu monga mwa malembo”.Marko 16:19; “Pamenepo Ambuye Yesu atathakulankhula nawo analandiridwa kumwambanakhala padzanja lamanja la Mulungu”.Machitidwe 17:31; “Chifukwa anapangira tsikulimene adzaweruza dziko lokhalamo anthum’chilungamo, ndi munthu amene anamuikiratu;napatsa anthu onse chitsimikizo, pameneanamuukitsa Iye kwa akufa’.

7

Page 8: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

9. NTCHITO YA MZIMU MUCHIPULUMUTSOFUNSOFUNSO 29.29. KodiKodi timatengatimatenga nawonawo gawogawobwanjibwanji kuku chiwombolochiwombolo chimenechimeneKhristuanatibweretsera?Khristuanatibweretsera?YANKHO. Ife timatenga nawo gawokuchiwombolochi pamene Mzimu wakeWoyera akhalamwa ife.Yohane 1:12; “Koma onse amene anamulandira Iye,anapatsa mphamvu kwa iwo yakukhala ana aMulungu, kwa iwotu akukhulupirira dzina lake”.Tito 3: 5,6; “Zosati zochokera ntchito zachilungamo zimene tidachita ife, koma monga mwachifundo chake anatipulumutsa ife, mwakutsukakwa kubadwanso ndi makonzedwe a MzimuWoyera, amene anatsanulira pa ife mochulukiramwa yesu Khristu Mpulumutsi wathu’.

FUNSOFUNSO 30.30. KodiKodi MzimuMzimu WoyeraWoyeraamatibweretseraamatibweretsera bwanjibwanji chiwombolochiwombolo chachaKhristu?Khristu?YANKHO. Mzimu Woyeraamatibweretsera chiwombolo cha Khristukupyolera mu chikhulupiriro cha ntchitocha mwa ife, kutiluzanitsa ife kwa Khristummaitanidwe athu.Aefeso 2:8; “Pakuti muli opulumutsidwa ndichisomo chakuchita mwachikulupiriro, ndipo ichindi chosachokera kwa inu chili mphatso yaMulungu”. Aefeso 3:17; “Kuti Khristu akhalechikhalire m’mitima yanu; kuti ozika mizu, ndiotsendereka mchikondi”. 1 Akorinto 1:9; “Mulunguali okhulupirika amene munaitanidwa kwa Iye,kuchiyanjano cha Mwana wake Yesu Khristu,Ambuye wathu”.

FUNSOFUNSO 31.31. KodiKodi maitanidwemaitanidwe enienienieni ndindichiyani?chiyani?YANKHO. Maitanidwe enieni ndi ntchitoya Mzimu Woyera wa Mulungu pameneatitsimikizira ife za machimo athu ndimazunzo pakutiunikira ife m’maganizo,mchidziwitso cha Khristu ndi kukonzansochifuniro chathu. Iye amatikakamizandikutipangitsa ife kufungatira YesuKhristu wopatsidwa kwa ife mwaulere waUthenga Wabwino.

2 Timoteo 1:19; “Amene anatipulumutsa ifenatiitana ife ndi maitanidwe oyera, simonga mwantchito zathu, komatu monga mwa chitsimikizommitima cha Iye Yekha, chi chisomo chopatsikakwa ife mwa Khristu Yesu zisanayambe nthawizoyamba”. Machitidwe 2: 37; “Koma pameneanamva ichi, analaswa mtima, natitu kwa Petro ndiatumwi enawo, tidzachita chiyani, amuna inuabale?” Ezekieli 36:26; “Ndipo ndidzakupatsanimtima watsopano ndi kulonga mkati mwanu, ndipondidzachotsa mtima wa mwala mthupindikukupatsani mtima wa mnofu”. Yohane 6:44-45;“Kulibe m’modzi akhoza kudza kwa Ine, koma ngatiAtate wondituma Ine amkoka iye, ndipo Inendidzamuukitsa iye tsiku lomaliza. Chalembedwamwa aneneri, ndipo adzakhala onse ophunzitsidwandi Mulungu. Yense amene adamva kwa Atatenaphunzira , adza kwa Ine”.

10. PHINDU LA CHIPULUMUTSOM’MOYO UNOFUNSOFUNSO 32.32. KodiKodi palipali phinduphindu lanjilanji limenelimeneoitanidwa amapeza mmoyooitanidwa amapeza mmoyo uno?uno?YANKHO. Phindu limene iwo amapezam’moyo uno ndi kulungamitsidwa kukhalaMwana wa Mulungu ndi kuyeretsedwa ndizina zambiri zabwino zimawatsatira iwo.Aroma 8:30; “Ndipo amene Iye anawalamuliratu,iwo anawaitananso; ndimo Iwo amene Iyeanawaitana, iwowa anawayesanso olungama; ndiiwo amene Iye anawayesa olungama, iwowaanawapatsanso ulemerero”. Aefeso 1:5; “ Pakuti ichimuchidziwe kuti wadama yense kapena wachidetsokapena wosirira, amene apembedza mafano, alibecholowa muufumu wa Khristu ndi Mulungu’. IAkorinto 1:30; “ Koma kwa Iye muli inu mwaKhristu Yesu, amene anayesedwa kwa ife nzeru yakwa Mulungu, ndi chilungamo ndi chiyeretso ndichiwombolo.

FUNSOFUNSO 33.33. KodiKodi kulungamitsidwakulungamitsidwa ndindichiyani?chiyani?YANKHO. Kulungamitsidwa ndimphamvu ya chisomo chaulere chaMulungu, imene Iye amatikhululukiramachimo athu onse, ndikutiyesa ifeolungama pamaso pake mwachilungamocha Khristu choikidwa mwa ife, ndiponsocholandiridwa mwa chikhulupiriro basi.

8

Page 9: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

Aefeso 1:7; “ Tiri ndi maomboledwe mwa mwaziwake, chikhululukiro cha zochimwa monga mwakulemera kwa chisomo chake”. 2 Akorinto 5:21;“Ameneyo sanadziwa uchimo, anamyereserauchimo m’malo mwathu; kuti ife tikhale chilungamocha Mulungu mwa Iye”. Aroma 5:19; Pakuti mongandikusamvera kwa munthu m’modzi ambirianayesedwa ochimwa, chomwechonso ndikumverakwa m’modzi onse adzayesedwa olungama”.Agalatiya 2:16; “Koma podziwa kuti munthusayesedwa olungama pa ntchito ya lamulo komamwa chikhulupiriro cha Yesu Khristu, ifeditinakhulupirira kwa yesu Khristu, kuti tikayesedweolungama ndi ntchito ya lamulo”.

FUNSOFUNSO 34.34. KodiKodi kukhalakukhala mwanamwana wawaMulungu kukutanthauza chiyani?Mulungu kukutanthauza chiyani?YANKHO. Kukhala mwana wa Mulungukukutanthauza mphatso yachisomochaulere cha Mulungu, imenetimalandiridwa mgulu la ana a Mulungundikukhala ndi ufulu wonse pa cholowacha ana a Mulungu”.Yohane 1:12; “Ngati ndakuuzani za pansi pano,ndipo simukhulupirira, mudzakhulupirira bwanjingati nditakuuzani za kumwamba? Aroma 8:17; “Ndipo ngati ana, pomweponso olowa nyumba; indeolowa anzake a Khristu; ngatitu ife timva zowawapamodzi naye, kutit tikalandirenso ulemereropamodzi ndi Iye”.

FUNSO 35.FUNSO 35. Kodi chiyeretso ndi chiyani?Kodi chiyeretso ndi chiyani?YANKHO. Chiyeretso ndi ntchito yachisomo chaulere cha Mulungu imene ifetimakonzedwanso muchifaniziro chaMulungu pakufa mu uchimo ndikukhalamuchilungamo.2 Atesalonika 2:13 “Ndipo mwaichinso, ifensotiyamika Mulungu kosalekeza, kuti pakulandiramawu a Uthenga wa Mulungu, simunawalandiramonga mawu a anthu, komatu mawu a Mulunguamenenso achita mwa inu okhulupirira”. Aefeso4:24; “Nimuvale munthu watsopano, ameneanalengedwa monga mwa Mulungu, m’chilungamo,ndi m’chiyero cha choonadi”. Aroma 8:1 “Chifukwachake tsopano iwo akukhala mwa Khristu Yesu alibekutsutsidwa”.

FUNSOFUNSO 36.36. KodiKodi ndindi phinduphindu lanjilanji kuku moyomoyounouno limenelimene limabweralimabwera chifukwachifukwa chacha

kulungamitsidwa,kulungamitsidwa, kukhalakukhala mwanamwana wawaMulungu, ndi kuyeretsedwa?Mulungu, ndi kuyeretsedwa?YANKHO. Ku moyo uno phindu limenelimabwera chifukwa cha kulungamitsidwa,kukhala mwana wa Mulungu ndikuyeretsedwa ndi: Chitsimikizochachikondi cha Mulungu, mtendere wachikumbumtima, chimwemwe mwaMzimu Woyera, kukula mu chisomondikukhala wopirira mpaka kumapeto.Aroma 5: 1, 2, 5; “Popeza tsono tayesedwaolungama ndi chikhulupiriro, tikhala ndi mtenderendi Mulungu wa Ambuye wathu Yesu Khristu,amene ife tikhoza kulowa naye chikhulupiriromchisomo ichi mmene tirikuimamo; ndipotikondwera mchiyembekezo cha ulemerero waMulungu. Ndipo chiyembekezo sichichititsamanyazi, chifukwa chikondi cha Mulunguchinatsanulidwa m’mitima mwathu mwa MzimuWoyera, amene wapatsidwa kwa ife”. Miyambo4:18; “Koma mayendedwe a olungama akungakuunika kwa m’bandakucha, kunkabe kuwalakufikira usana woti mbe”. 1 Yohane 5:13; “Izindakulemberani kuti mudziwe kuti tili nazo izitazipempha kwa Iye”.

11. PHINDU LACHIPULUMUTSOUKATHA MOYO UNOFUNSOFUNSO 37.37. KodiKodi okhulupiriraokhulupirira akamwaliraakamwaliraamalandiraamalandira phinduphindu lanjilanji kuchokerakuchokera kwakwaKhristu?Khristu?YANKHO. Mizimu ya anthu okhulupiriraimalungamitsidwa mu chiyero ndipoimalowa mu ulemerero; ndipo matupi awoali chilumikizire ndi Khristu, amapumulam’manda kufikira kuuka kwa akufa.Ahebri 12:23; “Ndi kwa msonkhano wa onse ndiMpingo wa obadwa olembedwa oyambaolembedwa m’mwamba ndi kwa MulunguWoweruza wa onse, ndi kwa angwiro”. Afilipi 1:23;“Koma ndipanidwa nazo ziwiri, pokhala nachocholakalaka chakuchoka kukhala ndi Khristu ndikokwabwino koposatu”. 1 Atesalonika 4:14; “Pakutingati tikhulupirira kuti Yesu adamwalira, naukakoteronso Mulungu adzatenga pamodzi ndi Iye iwoakugona mwa Yesu”. Yesaya 57: 2; “Iye alowa mumtendere, iwo apuma pa mphasa zawo, yensewoyenda moongoka”. Yobu 19:26; “Ndipo khungu

9

Page 10: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

langa litaononongeka, pamenepo wopanda thupilanga, ndidzapenya Mulungu”.

FUNSOFUNSO 38.38. KodiKodi ndindi phinduphindu lanjilanji limenelimeneokhulupiriraokhulupirira adzalandiraadzalandira papa tsikutsikulamdzukiro?lamdzukiro?YANKHO. Pa mdzukiro okhulupiriraadzaukitsidwa kunka ku ulemereronadzavomerezedwa poyerandikuweruzidwa monga anthuosachimwa ndipo adzakhala mu mdalitsondi muchikondwerero chachikulu chaMulungu ku nthawi zonse.1 Akorinto 15:43; “Lifesedwa m’mnyozo liukitsidwam’ulemerero; liukitsidwa mu mphamvu”. Mateyu10:32; “Chifukwa chake yense ameneadzavomereza Ine pamaso pa anthu, Inensondidzamvomereza iye pamaso pa Atate wanga wakumwamba”. 1 Yohane 3:2; “Kuti mukumbukiremawu onenedwa kale ndi aneneri oyera ndi lamulola Ambuye ndi Mpulumutsi, mwa atumwi anu”. 1Atesalonika 4:17; “Pamenepo ife okhala ndi moyo,otsalafe, tidzakwatulidwa nawo pamodzim’mitambo, kukakomana ndi Ambuyemumlengalenga, ndipo potero tidzakhala ndiAmbuye nthawi zonse”.

GAWO LACHIWIRI: ZIMENE TIYENERAKUMACHITA1. MALAMULO A CHIKHALIDWEFUNSOFUNSO 39.39. KodiKodi udindoudindo wawa munthumunthu kwakwaMulungu ndi wotani?Mulungu ndi wotani?YANKHO. Udindo wa munthu kwaMulungu ndiye kumvera chifuniro chake.Mika 6:7; “Kodi Yehova adzakondwera nazo nkhosazamphongo zikwi khumi? Kodi ndipereke mwanawanga woyamba chifukwa chakulakwa, chipatsocha thupi langa chifukwa cha kuchimwa kwa moyowanga?

FUNSOFUNSO 40.40. KodiKodi poyambapoyamba MulunguMulunguanaululaanaulula chiyanichiyani kwakwa munthumunthu palamulopalamulo lalakumverakumvera Iye?Iye?YANKHO. Mulungu analamula munthukumvera chilamulo chake.Aroma 2: 14-15; “Pakuti pamene anthu amitunduakukhala opanda lamulo, amachita mwa okha za

lamulo, omwewo angakhale alibe lamulo,adzakhalira okha ngati lamulo; popeza iwo aonetsantchito ya lamulolo yolembedwa m’mitima yao,ndipo chikumbumtima chao chichitiranso umbonipamodzi nawo, ndipo maganizo awo wina ndimzake anenezana kapena akanirana”.

FUNSOFUNSO 41.41. KodiKodi chilamulochilamulotingachimvetse kuchokera ku chiyani?tingachimvetse kuchokera ku chiyani?YANKHO. Chilamulo tingachimvetsebwino pa malamulo khumi a Mulungu.Deutronomo 10:4; “Ndipo analembera pamagomemonga mwa malembedwe oyamba, mawukhumiwo amene Yehova anena ndi inu m’phirimo,ali pakati pa moto tsiku la kusonkhanako ndipoYehova anandipatsa awa. Mateyu 19: 17; “NdipoIye anati kwa iye, undifunsiranji za chinthuchabwino? Alipo m’modzi ndiye wabwino, komangati ufuna kulowa m’moyo sunga malamulo”.

FUNSOFUNSO 42.42. KodiKodi malamulomalamulo khumikhumiamangidwa pa chiyani?amangidwa pa chiyani?YANKHO. Malamulo khumi amangidwapa izi: Kukonda Ambuye Mulungu ndimtima wathu wonse, moyo wathu wonse,mphamvu zathu zonse ndi nzeru zathuzonse ndi kukonda mnzathu mongatidzikondera ife eni.Mateyu 22:37, 39, 40; “Ndipo Yesu anati kwa iye,uzikonda Ambuye Mulungu wako ndi mtima wakowonse, ndi moyo wako wonse, ndi nzeru zakozonse. Ndipo lachiwiri lolingana nalo ndi ili:uzikonda mzako monga udzikondera iwe mwini.Pamalamulo awa awiri mpokolowekapo chilamulochonse ndi aneneri.

FUNSOFUNSO 43.43. KodiKodi maumau otsogoleraotsogolera kukumalamulo khumi ndi otani?malamulo khumi ndi otani?YANKHO. Mau otsogolera kumalamulokhumi ndi awa: Ine ndine Yehova Mulunguwako amene ndinakutulutsa iwe kudzikola Aiguputo munyumba ya ukapolo.Exsodo 20: 2 “Ine ndine Yehova Mulungu wako.Amene ndinatulutsa iwe ku dziko la Aigupto,kunyumba ya ukapolo.

FUNSOFUNSO 44.44. KodiKodi mawumawu otsogoleraotsogolera kukuMalamulo khumi akutiphunzitsa chiyani?Malamulo khumi akutiphunzitsa chiyani?YANKHO. Mau otsogolera ku Malamulokhumi a Mulungu amatiphunzitsa kuti

10

Page 11: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

popeza Mulungu ndi Ambuye ndiMulungu wathu ndiponso ndi mombolowathu, kotero kuti tiri oyenera kusungamalamulo ake onse.Deutronomo 11:1; “Chifukwa chake mudzikondaYehova Mulungu wanu, ndi kusunga chilangizochake, ndi malemba ake, masiku onse” Luka 1:74-75; “Kutipatsa ife kuti titalanditsidwa ku dzanjala adani athu, tidzamtumikira Iye, opanda mantha.M’chiyero ndi mchilungamo pamaso pake, masikuathu onse.

GAWO LOYAMBA LA MALAMULO2. LAMULO LOYAMBAFUNSOFUNSO 45.45. KodiKodi lamulolamulo loyambaloyamba ndindilotani?lotani?YANKHO. Lamulo loyamba ndi limenelimati: Usakhale nayo milungu ina komaIne ndekha.FUNSOFUNSO 46.46. KodiKodi mulamulomulamulo loyambaliloyambaliakufuna chiyani?akufuna chiyani?YANKHO. Mulamulo loyambali akufuna ifekudziwa ndi kuvomereza kuti MulunguYekha ndiye Mulungu woona ndi Mulunguwathu ndipo timupembedze ndikumulemekeza Iye moyenera.1 Mbiri 28:9; “Ndipo iwe Solomo mwana wangaumdziwe Mulungu wa atate wako, umtumikire ndimtima wangwiro ndi moyo waufulu pakuti Yehovaasanthula mitima yonse, nazindikira zolingalirazonse za maganizo. Ukamfunafuna Iye udzampeza,koma ukamsiya Iye adzakusiya kosatha”. Miyambo3:6; “Umlemekeze m’njira zako zonse, Ndipo Iyeadzaongola mayendedwe ako.”

FUNSOFUNSO 47.47. KodiKodi chimenechimene chikuletsedwachikuletsedwamu lamulo loyamba ndi chiyani?mu lamulo loyamba ndi chiyani?YANKHO. Mulamulo loyambachikuletsedwa ndi kukhala kopembedzamilungu ina.Masalimo 14:1; “Wauchitsiru amati mu mtimamwake kulibe Mulungu. Achita zovunda, achitantchito zonyansa, kulibe wakuchita bwino”. Mateyu4:10; “Pomwepo Yesu ananena kwa Iye, ChokaSatana, pakuti kwalembedwa, Ambuye Mulunguudzamgwadira, ndipo Iye yekha udzamlambira”.Aroma 1:25; “Amenewo anasandutsa choonadi cha

Mulungu chabodza napembedza natumikiracholengedwa ndi kusiya Wolengayo, ndiyewolemekezeka nthawi yosatha. Amen”.

FUNSOFUNSO 48.48. KodiKodi makamakamakamaka tikuphunziratikuphunzirachiyanichiyani mulamulomulamulo iliili loyambaloyamba mumu mawumawu otioti“Koma Inde Ndekha”?“Koma Inde Ndekha”?YANKHO. Mau oti koma Ine ndekha,akutiphunzitsa ife kuti Mulungu ameneamaona zonsesakondwera pamene ifetipembedza milungu ina.Masalimo 44: 20-21; “Tikadaiwala dzina laMulungu wathu, ndi kutambasulira manja athu kwamulungu wachilendo, Mulungu sakadasanthula ichikodi? Pakuti adziwa zinsinsi za mtima.”

3. LAMULO LACHIWIRIFUNSO 49.FUNSO 49. Kodi lamulo lachiwiri ndiKodi lamulo lachiwiri ndi liti?liti?YANKHO. Lamulo lachiwiri ndi ili:usadzipangire iwe wekha fano losemakapena chifaniziro chilichonse cha zinthuza mthambo lakumwamba kapena zamdziko lapansi kapena za m’madzi apansipa dziko; usazipembedzere izo,usazitumikire izo; chifukwa Ine YehovaMulungu ndiri Mulungu wansanjewakulanga ana chifukwa cha atate awo,kufikira m’badwo wachitatu ndi wachinayikwa iwo amene akudana ndi Ine;ndikuwachitira chifundo anthu zikwizikwia iwo amene akondana ndi Ine, nasungamalamulo anga.FUNSOFUNSO 50.50. KodiKodi mulamulomulamulo lachiwirilachiwirichikufunika ndi chiyani?chikufunika ndi chiyani?YANKHO. Mulamulo lachiwiri chikufunikandi kulandira, kutsatira ndi kusungakwathunthu zonse zokhuza chipembedzondi malamulo ake monga mmeneMulungu anasonyezera m’Mawu ake.Mateyu 28: 20; “Ndikuwaphunzitsa asunge zinthuzonse zimene ndinakulamulirani inu; ndipo onani,Ine ndiri pamodzi ndi inu masiku onse, kufikirachimaliziro cha nthawi ya pansi pano”.Deutronomo 12:32 “Chilichonse ndikuuzani,

11

Page 12: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

muchisamalire kuchichita musamaonjezako kapenakuchepetsako”.

FUNSOFUNSO 51.51. KodiKodi mulamulomulamulo lachiwirilachiwirichimene chili kuletsedwa ndi chiyani?chimene chili kuletsedwa ndi chiyani?YANKHO. Lamulo lachiwiri likuletsakupembedza Mulungu m’mafano kapenanjira ina iliyonseimene siinatchulidwe muMawu ake.Deutronomo 4:15; “Potere dzichenjerani nawomoyo wanu ndithu, popeza simunapenyamafanidwe konse tsikuli Yehova ananena ndi inum’Horebe, ali pakati pa moto. Kuti mungadziipsendi kudzipangira fano losema lakunga chifanizirochiri chonse, mafanidwe a mwamuna kapenamkazi”. Mateyu 15: 9; “Koma andilambira Inekwachabe, ndi kuphunzitsa maphunzitso,malangizo a anthu.

FUNSOFUNSO 52.52. KodiKodi ndindi mfundomfundo zotanizotanizimene zikupezeka mu lamulo lachiwiri?zimene zikupezeka mu lamulo lachiwiri?YANKHO. Mulamulo lachiwirimukupezeka mfundo izi kwa ife, umwiniwa Mulungu , kwa ife ndi chidwi chimeneali nacho kuchipembedzo chake.Masalimo 95: 3; “Pakuti Yehova ndiye Mulunguwamkulu ndi mfumu yaikulu yoposa milunguyonse”. Exsodo 34:14; “ Pakuti musalambireMulungu wina, popeza Yehova dzina lake ndiyeWansanje, ali Mulungu wansanje”.

4. LAMULO LACHITATUFUNSOFUNSO 53.53. KodiKodi lamulolamulo lachitatulachitatu ndindilotani?lotani?YANKHO. Lamulo lachitatu ndi ili:Usatchule dzina la Yehova Mulungu wakepachabe; chifukwa Yehova sadzamuyesaiye wosachimwa, amene atchula pachabedzina lakelo.FUNSOFUNSO 54.54. KodiKodi chikufunikachikufunika ndindi chiyanichiyanimu lamulo lachitatu?mu lamulo lachitatu?YANKHO. Lamulo lachitatu likufunachiyero ndi ulemu pogwiritsa ntchito dzinala Mulungu, Maudindo ake, Mau ake ndiNtchito zake.

Masalimo 29:2; “Perekani ulelemerero kwa Yehovamwa dzina lake, gwadirani Yehova moyera ndimokometsetsa”. Mlaliki 5:1; “Samalira phazi lakopopita ku nyumba ya Mulungu; pakuti kuyandikirakumvera kupambana kupereka nsembe za zitsiru;pakuti sizizindikira kuti zirikuchimwa”. Yobu 36:24; “Kumbukira kuti mukuze ntchito zake zimeneanaziyimbira anthu”.

FUNSOFUNSO 55.55. KodiKodi chikuletsedwachikuletsedwa ndindichiyani mu lamulo lachitatu?chiyani mu lamulo lachitatu?YANKHO. Mulamulo lachitatu akuletsakugwiritsa ntchito mosayenera ndimonyoza chinthu china chirichonsechimene Mulungu adzionetsera Yekha.Malaki 2:2; “Mukapanda kumvera, mukapandakuliika mumtima mwana, kupatsa dzina langaulemerero, ati Yehova wamakamu,ndidzakutumizirani temberero, ndi kutembereramadalitso anu; inde, ndawatemberera kale chifukwasimuliika mu mtima” Mateyu 5:34-35; “ Koma Inendinena kwa inu, Musalumbire konse, kapenakuchula kumwamba, chifukwa kuli chimpando chaMulungu. Kapena kuchula dziko lapansi, chifukwaliri popondapo mapazi ake; kapena kutchulaYerusalemu, chifukwa kuli mzinda wa Mfumuyaikurukuru”.

FUNSOFUNSO 56.56. KodiKodi ndindi mfundomfundo yotaniyotani imeneimeneikupezeka mulamulo lachitatu?ikupezeka mulamulo lachitatu?YANKHO. Mfundo imene ikupezekamulamuloli ndi yoti ngakhale anthuophwanya lamuloli angazembe chilangocha anthu, iwo sangazembe chilangochachilungamo cha Ambuye Mulunguwathu.Deuteronomo 28: 58-59; “Mukapanda kusamalirakuchita mau onse a chilamulo ichi olembedwam’buku ili, kuopa dzina ili la ulemerero ndi loopsa,ndilo YEHOVA MULUNGU WANU; Yehovaadzachita miliri yanu ndi ya ana anu ikhaleyodabwitsa, miliri yaikulu ndi yokhalitsa, ndinthenda zoipa ndi zokhalitsa”.

5. LAMULO LACHINAYIFUNSOFUNSO 57.57. KodiKodi lamulolamulo lachinayilachinayi ndindilotani?lotani?YANKHO. Lamulo lachinayi ndi ili:Udzikumbumbikira tsiku la Sabata likhalelopatulika. Mmasiku asanu ndi limodzi

12

Page 13: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

udzigwira ndikumaliza ntchito zako zonse;koma tsiku Lachisanu ndi Chiwiri ndiloSabata la Yehova Mulungu wako;Usagwire ntchito iliyonse, kapena iwewekha, kapena mwana wakowamwamuna, kapena mwana wako wamkazi, kapena wantchito wakowamwamuna, kapena wantchito wakowamkazi, kapena nyama zako, kapenamlendo amene ali m’mudzi mwako;chifukwa masiku asanu ndi limodziYehova anamaliza za kumwamba ndizapansi, ndi Nyanja, ndi zinthu zilim’menemo, napumula tsiku lachisanu ndichiwiri; chifukwa chake Yehova anadalitsatsiku la Sabata kuti likhale lopatulika.FUNSOFUNSO 58.58. KodiKodi chifunikachifunika ndindi chiyanichiyanimulamulo lachinayi?mulamulo lachinayi?YANKHO. Mulamulo lachinayi chifunikandi kusunga chiyero kwa Mulungu kunthawi zonse zoikika zimene Iyewazisankha m’mawu ake; ndikusungam’masiku asanu ndi awiri kuti likhaleSabata lopatulika kwa Iye Yekha.Levitiko 19:30; “Muzisunga masabata anga,ndikuchitira ulemu malo anga opatulika; Ine ndineYehova”. Deutronomo 5:12; “Samalira lasabatalikhale lopaturika monga Yehova Mulungu wakoanakulamulira”.

FUNSOFUNSO 59.59. KodiKodi ndindi tsikutsiku litiliti mwamwa masikumasikuasanuasanu ndindi awiriawiri limenelimene MulunguMulungu anapatulaanapatulakuti likhale la Sabata?kuti likhale la Sabata?YANKHO. Kuchokera pachiyambi chadziko kufikira kuuka m’manda kwa YesuKhristu, Mulunguanasankha tsikulachisanu ndi chiwiri (tsiku Loweruka) kutilikhale Sabata; ndipo atauka Yesu Khristusabata linasintha kukhala tsiku loyambala pa Sabata (tsiku la Mulungu), ndipo izizitsatiridwe mpaka kutha kwa dziko.Genesis 2:3; “Mulungu ndipo anadalitsa tsikulachisanu ndi chiwiri naliyeretsa limenelo chifukwalimenelo adapuma ku ntchito yake yonse imeneMulungu anairenga ndikuyipanga”. Machitidwe

20:7; “Ndipo tsiku loyamba lasabata posonkhanaife, kunyema mkate; Paulo anawafotokozera mawu,popeza anati achoke m’mawa wake ndipo ananenachinenere kufikira pakati pa usiku”. Chivumbulutso1:10; “Ndinagwidwa ndi mzimu Tsiku la Ambuyendipo ndinamva kumbuyo kwanga mawu akulungati a lipenga.

FUNSOFUNSO 60.60. NangaNanga tsikutsiku lala SabataSabata liyeneraliyenerakuyeretsedwa bwanji?kuyeretsedwa bwanji?YANKHO. Tsiku la Sabata liyenerakuyeretsedwa pakupumula mchiyero tsikulonse lathunthu ngakhalenso ku ntchitozonse za dziko ndi zamasewero zimenetimazigwira masiku onse ndikugwiritsantchito nthawi yathu yonsemkupembedza Mulungu m’magulukapena mwamseri, kupatulapo ntchitozofunikira zokha ndi chifundo.Levitiko 23:3; “Masiku asanu ndi limodzi azigwirantchito, koma lachisanu ndi chiwiri ndilo sabatala kupumula, msonkhano wopatulika; musagwirantchito konse; ndilo sabata la Yehova mnyumbazanu zonse”. Mateyu 12: 11-12; “Koma Iye anatikwa iwo, Munthu ndani wa inu amene ali nkhosaimodzi, ndipo ngati idzagwa mdzenje tsiku laSabata kodi sadzaigwira ndi kuiturutsa? Nangakuposa nkotani chifukwa cha ichi nkolekeka kuchitazabwino tsiku la Sabata”?

FUNSOFUNSO 61.61. KodiKodi chikuletsedwachikuletsedwa ndindichiyani mu lamulo lachinayi?chiyani mu lamulo lachinayi?YANKHO. Mulamulo lachinayichikuletsedwa ndi kusachita kapenakusasamala pakugwirantchito zoyenera,ndi kuoononga tsikuli pa kungokhalakapena kuchita tchimo kapena kukhalandi maganizo osayenera, m’mawu mu ndimu ntchito zathu zonse.Yesaya 58:13-14; “Ukaletsa phazi lako pa Sabatandi kusiya kuchita kukondwera kwatsiku langalopatulika, ndi kuyesa Sabata tsiku lokondwalopatulika la Yehova, lolemekezeka, ndipoukalilemekeza ilo, osachita njira zako zokha,osafuna kukondwa kwako kokha, osalankhulamawu ako okha; pomwepo udzakondwa mwaYehova; ndipo Ine ndidzakuyendetsa pa misanje yadziko lapansi; ndipo ndidzakudyetsa cholowa chakholo lako Yakokobo; pakuti pakamwa pa Yehovapananenapo.”Malaki 1:13; “Kutinso, taonani,

13

Page 14: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

ncholemetsa ichi! Ndipo mwachipeputsa, atiYehova wa Makamu; ndipo mwabwera nazozofunkha, ndi zotsimphina, ndi zodwala;momwemo mubwera nayo nsembe; kodi ndiyenerakuilandira kudzanja lanu? Ati Yehova”. Ezekekieli23: 38; “Anandichitiranso ichi, anadetsa malo angaopatulika tsiku lomwelo, naipsa masabata anga”.

FUNSOFUNSO 62.62. KodiKodi ndindi mfundomfundo zotanizotanizimene zikupezeka mu lamulo lachinayili?zimene zikupezeka mu lamulo lachinayili?YANKHO. Mfundo zopezeka mu lamulolachinayi ndi izi: Mulungu akutilola ifemasiku asanu ndi limodzi kugwira ntchitozathu zonse, tsiku lachisanu ndi chiwiri nditsiku la Yehova, Iye akupereka chitsanzocha Iye mwini, Iye akudalitsa tsiku laSabata.Eksodo 31:15; “Agwire ntchito masiku asanu ndilimodzi, koma lachisanu ndi chiwiri ndilo Sabatalakupumula, lopatulika la Yehova; aliyense wogwirantchito tsiku la Sabata aphedwe ndithu”. Genesis2:3; “Mulungu anadalitsa tsiku la chisanu ndichiwiri naliyeretsa limenelo: Chifukwa limeneloanapuma kuntchito yake yonse imene Mulunguanailenga ndi Kupanga.

GAWO LACHIWIRI LAMALAMULO6. LAMULO LACHISANUFUNSO 63.FUNSO 63. Kodi lamulo lachisanu ndiKodi lamulo lachisanu ndi liti?liti?YANKHO. Lamulo lachisanu ndi ili:Udzilemekeza atate wako ndi amako; kutiachuluke masikuako mu dziko limeneAmbuye Yehova Mulungu wako akupatsaiwe.FUNSOFUNSO 64.64. KodiKodi chikufunikirachikufunikira ndindi chiyanichiyanimulamulo lachisanu?mulamulo lachisanu?YANKHO. Mulamulo lachisanuchikufunikira ndi kusunga ulemu, ndikuonetsa ntchito zoyenerakwa aliyensemolingana ndi udindo wake kayawachikullire, wachicheperekapenawofanana naye usinkhu.Akolose 3:20; “Ana inu mverani akubala inum’zonse, pakuti ichi Ambuye akondwera nacho”.

Aefeso 5:21; “Ndi kumverana wina ndi mnzakem’kuopa Khristu”.

FUNSOFUNSO 65.65. NangaNanga chikuletsedwachikuletsedwa ndindichiyani mulamulo lachisanu?chiyani mulamulo lachisanu?YANKHO. Chimene chikuletsedwamulamulo lachisanu ndi kusaperekaulemu ndikusaonetsantchito zoyenerakwa aliyense molingana ndi udindo wakendi pamalo ake.Aroma 13: 7; “ Perekani kwa anthu onse mangawaawo; msonkho kwa eni ake ansonkho; kulipira kwaeni ake kulipidwa; kuopa kwa eni ake a kuwaopa;ulemu kwa eni ake a ulemu”.

FUNSOFUNSO 66.66. KodiKodi mulamulomulamulo limenelilimenelitikupezamo mfundo yotani?tikupezamo mfundo yotani?YANKHO. Mfundo yaikulu mu lamulolachisanu ndi lonjezo la moyo wautali ndiwotukuka kwaanthu onse osunga ilondipo ngati atero mu ulemerero waMulungu.Aefeso 6: 2-3; “Lemekeza atate wako ndi amako(ndilo lamulo loyamba lokhala nalo lonjezano), kutikukhale bwino ndi iwe, ndi kuti ukhale wa nthawiyaikuru padziko”.

7. LAMULO LACHISANU NDICHIMODZI (6)FUNSOFUNSO 67.67. KodiKodi lamulolamulo lachisanulachisanu ndindichimodzi ndichimodzi ndi liti?liti?YANKHO. Lamulo lachisanu ndi chimodzindi ili: Usaphe.FUNSOFUNSO 68.68. KodiKodi chikufunikachikufunika ndindi chiyanichiyanimu lamulo lachisanu ndi chimodzi?mu lamulo lachisanu ndi chimodzi?YANKHO. Mulamulo lachisanu ndichimodzi chimene chikufunika ndikusunga moyo wathu ndimiyoyo ya anthuena.Masalimo 82: 3-4; “Weruzani osauka ndi amasiye;Weruzani molungama ozunzika ndi osowa.Pulumutsani osauka ndi aumphawi; alanditsenim’dzanja la oipa.

14

Page 15: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

FUNSOFUNSO 69.69. KodiKodi chikuletsedwachikuletsedwa ndindichiyanichiyani mulamulomulamulo lachisanulachisanu ndindi chimodzi?chimodzi?YANKHO. Mulamuloli chikuletsedwa ndikudzichotsera moyo wa ife eni kapenamoyo wa m’bale wathu mopandachilungamo kapena mu njira ina iliyonse.Machitidwe 16:28; “Koma Paulo anafuula ndi mauaakulu kuti usadzipweteka wekha, tonse tili muno”.Mateyu 5:22; “Koma Ine ndinena kwa inu kuti yensewokwiyira mbale wake wopanda chifukwaadzakhala wopalamula mlandu; ndipo ameneadzanena ndi mbale wake, Wopanda pake iwe,adzakhala wopalamula mlandu wa akuru: Komaamene adzati, chitsiru iwe: adzakhala wopalamulagehena wamoto”.

8. LAMULO LACHISANU NDICHIWIRI (7)FUNSOFUNSO 70.70. KodiKodi lamulolamulo lachisanulachisanu ndindichiwiri ndichiwiri ndi liti?liti?YANKHO. Lamulo lachisanu ndi chiwiri ndiili: Usachite chigololo.FUNSOFUNSO 71.71. KodiKodi chikufunikirachikufunikira ndindi chiyanichiyanimulamulo lachisanu ndi chiwiri?mulamulo lachisanu ndi chiwiri?YANKHO. Mulamulo lachisanu ndi chiwirichimene chikufunikira ndi kudziletsa kwaife eni, kulemekeza umunthu wa anzathumu mtima, m’malankhulidwe ndim’makhalidwe.2 Timoteo 2:22; “Koma thawa zilakolako zaunyamata, nusate chilungamo, chikhulupiriro,chikondi, mtendere pamodzi ndi iwo akuitana paAmbuye ndi mitima yoyera”. Aefeso 5: 11-12;“Ndipo musayanjane nazo ntchito za mdimazosabala kanthu, koma makamakanso mudzitsutse.Pakuti zochitidwa mtseri , kungakhale kuzinenakuchititsa manyazi”.

FUNSOFUNSO 72.72. KodiKodi chikuletsedwachikuletsedwa ndindichiyani mu lamulo lachisanu ndi chiwiri?chiyani mu lamulo lachisanu ndi chiwiri?YANKHO. Lamulo limeneli likuletsamalingaliro onse oipa, mawu achabe ndintchito zonse zosayenera.Mateyu 5:28; “Koma Ine ndinena kwa Inu, kutiyense wakuyang’ana mkazi kumkhumba,pamenepo watha kuchita naye chigololo mu mtimamwake”. Aefeso 5:4; “Kapena zonyasa, ndi

kulankhula zopanda pake, kapena zopusa zimenesiziyenera; koma makamaka chiyamiko”.

9. LAMULO LACHISANU NDICHITATU (8)FUNSOFUNSO 73.73. KodiKodi lamulolamulo lachisanulachisanu ndindichitatu ndichitatu ndi liti?liti?YANKHO. Lamulo lachisanu ndi chitatundi ili: UsabeFUNSOFUNSO 74.74. KodiKodi chikufunikachikufunika ndindi chiyanichiyanimu lamulo lachisanu ndi chitatu?mu lamulo lachisanu ndi chitatu?YANKHO. Lamulo lachisanu ndi chitatulikufuna ife kudzipezera chuma ndikatundu wina mu njira yoyenera komansoyachilungamo.Aefeso 4:28; “Wakubayo asabenso; komamakamaka agwiritse ntchito, nagwire ntchitoyokoma ndi manja ake, kuti akhale nachochakuchereza wosowa. Aroma 12:17;“Musabwezere munthu aliyense choipa.Ganiziranitu zinthu za ulemu pamaso pa anthuonse”.

FUNSOFUNSO 75.75. KodiKodi chikuletsedwachikuletsedwa ndindichiyani mulamulo lachisanu ndi chitatu?chiyani mulamulo lachisanu ndi chitatu?YANKHO. Chimene chikuletsedwamulamuloli ndi kudzitengera kwa ife tokhachuma kapena katundu wa anzathu munjira yopanda chilungamo.Miyambo 28:19; “Wolima munda wake zakudyazidzamkwanira; koma wokhota m’mayendedwe akeadzagwa posachedwa”. Machitidwe 20: 35;“Mzinthu zonse ndinakupatsani chitsanzo, chakutipogwiritsa ntchito, kotero muyenera kuthandizaofoka ndikukumbuka mau a Ambuye Yesu, kutianati Yekha, Kupatsa kutidalitsa koposa kulandira”.Miyambo 21:6 “Kupata chuma ndi lilime lonamandiko nkhungu yoyendayenda ngakhale misamphaya imfa”.

10. LAMULO LACHISANU NDICHINAYI (9)FUNSOFUNSO 76.76. KodiKodi lamulolamulo lachisanulachisanu ndindichinayi ndichinayi ndi liti?liti?YANKHO. Lamulo lachisanu ndichinayindi ili: Usamnamizire mzako.

15

Page 16: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

FUNSOFUNSO 77.77. KodiKodi chikufunikirachikufunikira ndindi chiyanichiyanimulamulo lachisanu ndi chinayi?mulamulo lachisanu ndi chinayi?YANKHO. Lamulo lachisanu ndi chinayilikutipempha ife kusunga ndi kukwezachoonadi pakatipathu ndi kuchitiranaumboni.Zekariya 8:16; “Izi ndizo muzichite; weruzanizoona ndi chiweruzo cha mtendere m’zipata zanu”.Miyambo 14: 5, 25; “Mboni yokhulupirikasidzanama, koma mboni yonyenga imalankhulazonama. Mboni yoona imalanditsa miyoyo; komawolankhula zonama angonyenga”.

FUNSOFUNSO 78.78. KodiKodi chikuletsedwachikuletsedwa ndindichiyani mulamulo lachisanu ndichinayi?chiyani mulamulo lachisanu ndichinayi?YANKHO. Mulamulo lachisanu ndichinayichimene chikuletsedwa ndi chinachilichonse choipitsa choonadi kapenakudzionongetsa ife tokha komanso mainaabwino a anzathu.Masalimo 15:3; “Amene sasinjirira ndi lilime lake,sachitira nzake choipa. Ndipo satola mseche pamnasi wake”. Aroma 3:13; “Mmero mwao mulimanda apululu, ndi lilime lawo amanyenga; Ululuwa mamba uli pa milomo yawo”. Aefeso 4:31;“Chiwawo chonse, ndi kupsa mtima, ndi mkwiyo,ndi chiwawa, ndi mwano zichotsedwe kwa inu,ndiponso choipa chonse.

11. LAMULO LAKHUMIFUNSO 79.FUNSO 79. Kodi lamulo lakhumi ndiKodi lamulo lakhumi ndi liti?liti?YANKHO. Lamulo lakhumi ndi limenelimati: usasirire nyumba yake ya mzako,usasirire mkazi wake wa mnzako, kapenawantchito wake wa mwamuna, kapenawantchito wake wa mkazi, kapenang’ombe yake kapena bulu wake, kapenakanthu kalikonse kamzako.FUNSOFUNSO 80.80. KodiKodi chikufunikirachikufunikira ndindi chiyanichiyanimulamulo la khumi?mulamulo la khumi?YANKHO. Lamulo la khumi likutiphunzitsaife kukhala okwanitsidwa ndikukhala ndimtima wolemekeza katundu wa anthu.1 Timoteo 6:8; “Koma pokhala nazo zakudya ndizofunda , zimenezi zitikwanire. Ahebri 13:5;“Mtima wanu ukhale osakonda chuma; zimene mulinazo zikukwanireni; pakuti iye anati, sindidzakusiya

konse, kungakhale kukutaya, sindidzakutayandithu”.

FUNSOFUNSO 81.81. KodiKodi chikuletsedwachikuletsedwa ndindichiyani mulamulo la khumi?chiyani mulamulo la khumi?YANKHO. Lamulo lakhumi likutiletsa ifekukhala osakwanitsidwa pa zinthu zimenetili nazo, kuchitira nsanje kapena kuipidwandi zinthu zabwino za anzathu.Agalatiya 5:26; “Tisakhale odzikuza, osutsana,akuchitirana njiru”. Luka 12:15; “Ndipo Iye anatikwa iwo, Yang’anirani, mudzisungire kupewamsiriro uliwonse; chifukwa moyo wake wa munthusulingana ndi kuchuluka kwa zinthu zake ali nazo”.

12. CHILANGO CHOPHWANYALAMULO LA MULUNGUFUNSOFUNSO 82.82. KodiKodi palipali munthumunthu aliyensealiyenseameneamene angasungeangasunge mwangwiromwangwiro malamulomalamuloa Mulungu?a Mulungu?YANKHO. Palibe ndi m’modzi yemweangathe kusunga malamulo a Mulungumwangwiro m’moyo uno, pakuti munthuamachimwa nthawi ndi nthawim’maganizo, m’mawu ndi m’machitidwe.Mlaliki 7:20; “Pakuti palibe wolungama pansi pano,amene achita zabwino osachimwa”. Masalimo14:3; “Anapatuka onse; pamodzi anabvunda mtima;palibe wakuchita bwino ndi mmodzi yense”.

FUNSOFUNSO 83.83. KodiKodi machimomachimo ophwanyaophwanyamalamulomalamulo aa MulunguMulungu ndindi ofananaofanana kuopsyakuopsyakwawo?kwawo?YANKHO. Machimo ena ndi oopsyakuposa ena pamaso pa Mulungu.Luka 12: 47-48; “Ndipo kapolo uyo, wodziwachifuniro cha Ambuye wake, ndipo sanakonza ndikusachita zonga za chifuniro chakecho,adzakwapulidwa mikwapulo yambiri. Koma Iyeamene sanadziwa, ndipo anazichita zoyeneramikwapulo, adzakwapulikwa pang’ono.

FUNSOFUNSO 84.84. KodiKodi tchimotchimo lirilonselirilonselimayenera chiyani?limayenera chiyani?YANKHO. Tchimo lirilonse limayeneraMkwiyo ndi Temberero la Mulungum’moyo uno komanso umene ulikudza.

16

Page 17: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

Aroma 6:23; “Pakuti mphoto yake ya uchimo ndiimfa”. Mateyu 25: 41; “Pomwepo adzanena kwakwa iwo a ku dzanja lamanzere, Chokani kwa Ineotembereredwa inu, ku moto wa nthawi zonsewokolezedwera mdierekezi ndi a mithenga ake”.

13. NJIRA YA CHIPULUPUMUTSOFUNSOFUNSO 85.85. KodiKodi MulunguMulungu akufunaakufuna tichitetichitechiyanichiyani kutikuti tipewetipewe mkwiyomkwiyo ndindi tembererotembereromalingana ndi tchimo lathu?malingana ndi tchimo lathu?YANKHO. Kuti tipewe mkwiyo nditemberero malingana ndi machimo athu,Mulungu akufuna ife tikhale ndichikhulupiriro mwa Yesu Khristu, moyowakulapa, ndikugwira njira zonsezachiombolo zimene Yesu anatiululira.Machitidwe 20: 21; “Ndikuchira umboni a Yudandi a Helene wa kutembenuka mtima kulinga kwaMulungu ndi chikhulupiriro cholinga kwa Ambuyewathu.

FUNSOFUNSO 86.86. KodiKodi chikhulupirirochikhulupiriro mwamwa YesuYesuKhristu ndi chiyani?Khristu ndi chiyani?YANKHO. Chikhulupiriro mwa YesuKhristu ndi chisomo cha chipulumutsochathu, chimene timalandira ndikutsamira pa Iye yekha kutitipulumutsidwe, monga anadziperekerakwa ife mu uthenga wabwino.Yohane 3:16; “Pakuti Mulungu anakonda dzikolapansi kotero anatuma Mwana Wake WobadwaYekha, kuti wokhulupirira Iye asataike koma akhalenawo moyo wosatha”. Machitidwe 4:12; “Ndipopalibe chipulumutso mwa wina yense, pakuti palibedzina lina pansi pathambo lakumwamba,lopatsidwa mwa anthu, limene tiyenerakupulumutsidwa nalo”.

FUNSOFUNSO 87.87. KodiKodi moyomoyo wakulapawakulapa ndindichiyani?chiyani?YANKHO. Moyo wakulapa ndi chisomochopulumutsa chochitika pamenewochimwa wazindikira tchimo lake ndichifundo cha Mulungu mwa Khristu ndikumva chisoni ndi kudana ndi tchimolake, ndikutembenukira kwa Mulungumotsimikizika ndikuyamba kumvera Iye.

Luka 13:3; “Ndinena kwa inu, Iaitu; koma ngatiinu simutembenuka mtima, mudzaonongeka nonsemomwemo”. Luka 18:13; “Koma wamsonkhoyoalikuima patali sanafuna kungakhale kukweza masokumwamba, komatu anaziguguda pachifuwa pakenanena, Mulungu, mundichitire chifundo, inewochimwa”.

FUNSOFUNSO 88.88. KodiKodi ndindi njiranjira zitiziti zimezime KhristuKhristuamationetsera ife ubwino wa chiombolo?amationetsera ife ubwino wa chiombolo?YANKHO. Njira zimene Khristuamationetsera ife ubwino wa chiombolondi kudzera m’malamulo ake,makakamaka m’mawu, masakaramentindi pemphero; ndipo izi zonse zimagwirantchito ku chipulumutso cha osankhika.Machitidwe 2:42; “Ndipo anali chikhalirem’chiphunzitso cha atumwi ndi m’chiyanjano,m’kunyema mkate ndi mapemphero. 2 Timoteo3:15; “Ndikuti kuyambira ukhanda wako wadziwamalembo opatulika, okhoza kukupatsa nzerukufikira chipulumutso, mwa chikhulupiriro chamwa khristu Yesu”.

14. BUKU LOPATULIKA (BAIBULO)NGATI NJIRA YA CHISOMOFUNSOFUNSO 89.89. KodiKodi MauMau amapangigwaamapangigwabwanjibwanji kukhalakukhala ndindi mphamvumphamvuyopulumutsa?yopulumutsa?YANKHO. Mzimu wa Mulunguumapangitsa kuwerenga kwa Mau aMulungu makamaka ulaliki, kukhala njirayotsimikizika ndiponso yotembenuziraochimwa pakuwaiika iwo mu chiyero ndimuchitonthozo, kupyolera muchikhulupiriro kufikira ku chipulumutso.Masalimo 19:7; “Zakumwamba zimalalikiraulemerero wa Mulungu; ndipo thambo lionetsantchito ya manja ake”. 2 Timoteo 3:16; “Lembaliri lonse adaliuzira Mulungu, ndipo lipindulitsa pachiphunzitso, chitsutsano, chikonzero, chilangizocha m’chipulumutso.

FUNSOFUNSO 90.90. NangaNanga mawumawuangawerengedweangawerengedwe ndindi kumvekakumveka bwanjibwanjikuti akhale ndi mphamvu yopulumutsa?kuti akhale ndi mphamvu yopulumutsa?YANKHO. Kuti mawuwa akhale ndimphamvu yopulumutsa tiyenera

17

Page 18: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

kumvetsetsa bwino pokonzekera ndipemphero, kuwalandira ndi chikhulupirirondi chikondi ndi kuwakhazikitsa m’mitimayathu ndikuwagwiritsa ntchito mmoyowathu.Masalimo 119:11; “Ndinawabisa mawu anu mumtima mwanga, kuti ndisalakwire Inu”. Ahebri 4:2;“Pakuti kwa ifenso walalikidwa uthenga wabwino,monganso kwa iwo; koma iwowa sanapindula nawomau omvekawo, popeza sanasanganizika ndichikhulupiriro mwa iwo amene adamva”.

15. MASAKARAMENTI NGATI NJIRAYACHISOMOFUNSOFUNSO 91.91. KodiKodi masakaramentimasakaramentiamakhala bwanji njira yachipulumutso?amakhala bwanji njira yachipulumutso?YANKHO. Masakaramenti amakhala njirayachipulumutso, osati mwa iwo wokha ayikapena amene awagwiritsa ntchito iwo,koma ndi mdalitso wa Khristu wokha, ndintchito ya Mzimu Woyera mwa iwo ameneawalandira ndi chikhulupiriro.1 Akorinto 3:7; “Chotero Sali kanthu kapenawookayo, kapena wothirirayo; koma Mulunguamene akulitsa”. 1 Akorinto 11:29; “Pakuti iyewakudya ndi wakumwa, adya namwa chiweruzirokwa iye yekha, ngati sazindikira thupilo”. 1 Petulo3:21; “Chimenechonso chifaniziro chakechikupulumutsani tsopano, ndicho ubatizo, kosatikutaya kwa litsiro lake la thupi, komatu funso lakela chikumbumtima chokoma cha Mulungu, mwakuuka kwa Yesu Khristu”.

FUNSOFUNSO 92.92. KodiKodi SakaramentiSakaramenti ndindichiyani?chiyani?YANKHO. Sakaramenti ndi lamulo loyeralokhazikitsidwa ndi Khristu, limenemukupyolera muzizindikiro zooneka,Khristu ndi ubwino wa Panganolatsopano, zimaonekera, kusindikizidwandi kutsatiridwa ndi okhulupirira.Genesis 17:10; “Ili ndi pangano langa limeneuzisunga pakati pa Ine ndi Iwe ndi mbewu zakozapambuyo pako; azidulidwa amuna onse amwainu”. Aroma 4:11; “Ndipo iye analandirachizindikiro cha mdulidwe, ndicho chosindikizachilungamo cha chikhulupiriro, chomwe iye analinacho asanadulidwe; kuti kotero Iye akhale kholo

la onse akukhulupirira, angakhale iwo sanadulidwa,kuti chilungamo chiwerengedwe kwa iwonso”.

FUNSOFUNSO 93.93. KodiKodi masakaramentimasakaramenti aaChipangano Chatsopano ndiChipangano Chatsopano ndi ati?ati?YANKHO. Masakaramenti a ChipanganoChatsopano ndi awa: Ubatizo ndiMgonero wa Ambuye.Mateyu 28:19; “Chifukwa chake mukani,phunzitsani anthu a mitundu yonse, ndi kuwabatizaiwo m’dzina la Atate, ndi la Mwana, ndi la MzimuWoyera”. Mateyu 26:26; “Ndipo pamene iwo analikudya, Yesu anatenga mkate, nadalitsa, naunyema;ndipo m’mene anapatsa kwa ophunzira, anati,Tengani, idyani; ichi ndi thupi langa”.

16. UBATIZOFUNSO 94.FUNSO 94. Kodi ubatizo ndi chiyani?Kodi ubatizo ndi chiyani?YANKHO. Ubatizo ndi sakaramenti limenemunthu amatsambitsidwa ndi madzim’dzina la Atate ndi la Mwana ndi laMzimu Woyera, chimene chiri chizindikirocha malowedwe athu kwa Khristu ndikulandira ubwino wa Chipangano chaChisomo ndikukhala ake a Ambuye.Mateyu 28:19; “Chifukwa chake mukani,phunzitsani anthu a mitundu yonse, ndi kuwabatizaiwo m’dzina la Atate, ndi la Mwana, ndi la MzimuWoyera”. Aroma 6:3; “Kapena kodi simudziwa kutiife tonse amene tinabatizidwa mwa Khristu Yesu,tinabatizidwa mu imfa yake?”

FUNSOFUNSO 95.95. KodiKodi ubatizoubatizo ungaperekedweungaperekedwekwakwa yani?yani?YANKHO. Ubatizo siuyenera kwa munthuwina aliyense amene ali kunja kwa mpingokufikira atavomereza chikukhulupirirochawo mwa Khristu ndi kumvera Iye;komanso ana popeza nawonso alichiwalo cha mpingo, ayenerakubatizidwa.Machitidwe 2:41; “Pamenepo iwo ameneanalandira mawu ake anabatizidwa; ndipoanaonjezedwa tsiku lomwelo anthu ngati zikwizitatu (3000)”. Machitidwe 2:39; “Pakuti lonjezanoliri kwa inu,, ndi kwa ana anu, ndi kwa onse akutali,onse amene Ambuye Mulungu wathu adzaitana”.

18

Page 19: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

17. MGONERO WA AMBUYEFUNSOFUNSO 96.96. KodiKodi mgoneromgonero wawa AmbuyeAmbuyendi chiyani?ndi chiyani?YANKHO. Mgonero ndi sakaramentilimene pakupereka ndi kulandira vinyomonga momwe Khristu anachitira, imfayake imaonetsedwa; ndipo olandirawosangolandira kuthupi, komamwachikhulupiriro amadya nawo thupi ndikumwa mwazi wake ndi ubwino wakewonse, ku moyo wawo wa uzimundikukula kwawo mu chisomo.1 Akorinto 10:16; “Chikho chadalitso chimenetidalitsa, sichiri chiyanjano cha mwazi wa Khristukodi? Mkate umene tinyema suli chiyanjano chathupi la Khristu kodi?” 1 Akorinto 11: 23; “Pakuti inendinalandira kwa Ambuye chimenenso ndinaperekakwa inu, kuti Ambuye Yesu usiku ujaanaperekedwa, anatenga mkate…”. Luka 22: 19-20;“Ndipo mmene anatenga mkate, nayamika,anaunyema nawapatsa, nanena, Ichi ndi thupilanga, lopatsidwa chifukwa cha inu; chitani ichichikumbukiro changa. Ndipo choteronso chikho,atatha mgonero, nanena, Chikho ichi ndi panganolatsopano m’mwazi wanga wothiridwa chifukwacha Inu”.

FUNSOFUNSO 97.97. KodiKodi chikufunikachikufunika ndindi chiyanichiyanikwakwa iwoiwo oyeneraoyenera kulandirakulandira mgoneromgonero wawaAmbuye?Ambuye?YANKHO. Chofunika kwa iwo oyenerakulandira mgonero wa Ambuye ndi kutiadziyese okha mu nzeru zawopakuzindikira thupi la Ambuye,chikhulupiriro chawo, kulapa kwawo,chikondi ndi kumvera kwatsopano, poopakuti ngati ali osayenera, akhozakudziitanira mkwiyo wa Mulungu kwa iwoeni.1 Akorinto 11: 28-29; “Koma munthu adziyeseyekha, ndikotero adye mkate, ndikumwera chikho.Pakuti iye wakudya, adya namwa chiweruziro kwayekha, ngati sazindikira thupilo”. 1 Akorinto 5:8;“Chifukwa chake tichita phwando sindichotupitsachakale, kapena ndi chotupitsa cha dumbo ndikuipa mtima, koma ndi mkate wosatupa wa kuonamtima ndi choonadi”.

18. PEMPHERO NGATI NJIRAYACHISOMOFUNSO 98.FUNSO 98. Kodi pemphero ndi chiyani?Kodi pemphero ndi chiyani?YANKHO. Pemphero ndikuperekazokhumba zathu kwa Mulungu ku zinthuzovomerezeka ndi chifuniro chake mudzina la Khristu,ndi pakulapa machimoathu ndi kuvomereza koyamika chifundochake.Mateyu 7:7; “Pemphani ,ndipo chidzapatsidwa kwainu; funani, ndipo mudzapeza; gogodani, ndipochidzatsegulidwa kwa inu”. Yohane 16: 23; “Indetu, Indetu ndinena kwa inu, ngati mudzapempha Atatekanthu, adzakupatsani inu mu dzina langa”. Afilipi4:6; “Musadere nkhawa konse, komatu muzonsendipemphero, ndi pembedzero, pamodzi ndichiyamiko zopempha zanu zidziwike kwaMulungu”.

FUNSOFUNSO 99.99. KodiKodi ndindi lamulolamulo lotanilotani limenelimeneMulunguMulungu waperekawapereka lotitsogoleralotitsogolera kukupemphero?pemphero?YANKHO. Mau onse a Mulungu am’Bukhu Lopatulika ndiwo atitsogolera ifem’pemphero; komanso pali lamulolapadera limene Khristu anaphunzitsaophunzira ake, limene litchedwaPemphero la Ambuye.1 Yohane 5:14; “Ndipo uku ndikulimbika mtimakumene tiri nako kwa Iye, kuti ngati tipemphakanthu monga mwa chifuniro chake,atimvera”.Mateyu 6:9; “Chifukwa chakepempherani inu chomwechi: Atate wathu waKumwamba, Dzina lanu liyeretsedwe, ….”.

19. PEMPHERO LA AMBUYEFUNSOFUNSO 100.100. KodiKodi maumau oyambiriraoyambirira papapempheropemphero lala AmbuyeAmbuye amatiphunzitsaamatiphunzitsa ifeifechiyani?chiyani?YANKHO. Mau oyambirira a pemphero laAmbuye oti: Atate wathu wakumwamba,amatiphunzitsa ife kusendeza chifupi ndiMulungu mkudzichepetsa konse,mchiyero ndi chitsimikizo monga ana kwaatate wawo, okhoza kutithandiza ife,

19

Page 20: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

ndikuti tikhoza kudzipempherera tokhandikupemphereranso anzathu.Mateyu 6:9; “Chifukwa chake pempherani inuchomwechi: Atate wathu wa Kumwamba, Dzinalanu liyeretsedwe, ….”. Aroma 8:15; “Pakuti inusimunalandira mzimu waukapolo, kuchitansomantha, koma munalandira Mzimu wa umwanaumene tifuula kuti Abba, Atate”.

FUNSOFUNSO 101.101. KodiKodi timapemphereratimapemphererachiyani mugawo loyamba?chiyani mugawo loyamba?YANKHO. Mugawo loyamba (limene liri:Dzina Lanu Liyeretsedwe)timapemphaMulungu kuti atipangitse ife ndi anzathukumulemekeza Iye mu zonse zimeneamazionetsera; kuti atiwonetse ulemererowake ku zinthu zake zonse.Masalimo 67: 3 “Anthu akuyamikeni, Mulungu;Anthu onse akuyamikeni. Aroma 11:36; “Chifukwazinthu zonse zichokera kwa Iye, zichitika mwa Iyendikufikira kwa Iye, kwa Iyeyo kukhale ulemererokunthawi zonse. Amen”.

FUNSOFUNSO 102.102. KodiKodi timapemphereratimapemphererachiyani mu chigawo chachiwiri?chiyani mu chigawo chachiwiri?YANKHO. Muchigawo chachiwiri(chimene chiri: Ufumu Wanu Udze),timapempherera kuti ufumu wa Satanauwonongedwe; ndi kuti ufumu wachisomo ukudzidwe mwa ife ndi enaotengedwa nawo momwemu, ndi kutiufumu wa ulemerero ufulumizidwe.Masalimo 68:1; “Auke Mulungu, abalalike adaniake; Iwonso akumuda athawe pamaso pake”.Masalimo 51:18; “Chitirani Ziyoni chokoma mongamwa kukondwera kwanu, mumange malinga amiyala a Yerusalemu”. Chibvumbulutso 22: 20; “Iyewakuchitira umboni izi, anena, Indetu ndidzansanga Ameni; Idzani Ambuye Yesu”.

FUNSOFUNSO 103.103. KodiKodi timapemphereratimapemphererachiyani mu chigawo chachitatu?chiyani mu chigawo chachitatu?YANKHO. Muchigawo chachitatu(chimene chiri: Kufuna kwanu kuchitidwemonga kumwamba chomwecho pansipano), timapempherera kuti Mulungumwa chisomo chake atipangitse ifekudziwa, kumvera, ndi kugonjera ku

chifuniro chake mu zinthu zonse, mongaalikuchitira angelo kumwamba.Masalimo 119:34; “Mundizindikiritse, ndipondidzasunga malamulo anu; Ndidzawasamalira ndimtima wanga wonse”. Mateyu 26: 39; “Ndipoanamuka patsogolo pang’ono, nagwa nkhope yakepansi, napemphera nati, Atate ngati nkutheka,chikho ichi chindipitirire Ine; koma simonga ndifunaIne koma Inu.

FUNSOFUNSO 104.104. KodiKodi timapemphereratimapemphererachiyani mu chigawo chachinayi?chiyani mu chigawo chachinayi?YANKHO. Muchigawo chachinayi(Chimene chiri: Mutipatse ife chakudyachathu chalero) timapempherera kuti:Kuchokera mu mphatso yaulere yaMulungu, tilandireko gawo la zinthuzabwino m’moyo uno, ndi kukondwerandi madalitso ake.Miyambo 30:8; “Mundichotsere kutali zachabe ndimabodza; musandipatse umphawi ngakhale chuma,mundidyetse zakudya zondiyenera”. Masalimo90:17; “Ndipo chisomo chake cha Yehova Mulunguwathu chikhale pa ife. Ndipo mutikhazikitsire ifentchito ya manja athu, inde ntchito ya manja athumuikhazikitse”.

FUNSOFUNSO 105.105. KodiKodi timapemphereratimapemphererachiyani muchigawo chachisanu?chiyani muchigawo chachisanu?YANKHO. Muchigawo chachisanu(Chimene chiri: Ndipo mutikhululukire ifezochimwa zathu monga ifensotiwakhululukira amangawa athu)timapemphelera kuti Mulungu mwaKhristu, atikhululukire zochimwa zathu;zomwe ife tikukakamizidwa kupempha,chifukwa mwa chisomo chake ife tilikuloledwa kukhululukira anzathukuchokera pansi pa mtima.Masalimo 51:1; “Mundichitire ine chifundoMulungu, monga mwakukoma mtima kwanu,monga mwa unyinji wa nsoni zokoma zanumufafanize machimo anga”. Mateyu 6: 14; “Pakutingati mukhululukira anthu zolakwa zawo,adzakhululukira inunso Atate wanuwakumwamba”.

20

Page 21: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

FUNSOFUNSO 106.106. KodiKodi timapemphereratimapemphererachiyanichiyani muchigawomuchigawo chachisanuchachisanu ndindichimodzi?chimodzi?YANKHO. Muchigawo chachisanu ndichimodzi (Chimene chiri: Musatitengereife kokatiyesa, koma mutipulumutse ifekwa woipayo), timapempherera kutiMulungu atichinjirize ife ku mayesero auchimo, kapena kutithandiza kutilanditsaife pamene tiyesedwa.Mateyu 26: 41; “Chezerani ndi kupemphera kutimungalowe mkuyesedwa; Mzimutu uli wakufakoma thupi liri lolefuka”. Masalimo 19:13;“Ndiponso muletse kapolo wanu pa zodzitama;zisachite ufumu pa ine: pamenepo ndidzakhalawangwiro, ndiwosachimwa cholakwa chachikuru.

FUNSOFUNSO 107.107. KodiKodi kutsirizakutsiriza kwakwapempheropemphero lala AmbuyeAmbuye kumatiphunzitsakumatiphunzitsa ifeifechiyani?chiyani?YANKHO. Matsiriziro a pemphero laAmbuye (amene ali: Pakuti wanu uli ufumu

ndi mphamvu ndi ulemerero, wanthawizonse Amen) , akutiphunzitsa ife kukhalandi chilimbikitso mu pemphero la Ambuyelokha basi; ndi m’mapemphero athuolemekeza iye, potchula ufumu,mphamvu ndi ulemerero kwa Iye. Ndipopakuchitira umboni pakhumbo lathu, chichitsimikizo chofuna kumvetseredwa,tikuti Amen.1 Mbiri 29:11,13; “Ukulu ndi mphamvu ndiulemelero ndi kulakika, ndi chifumu ndi zanuYehova; pakuti zonse zam’mwamba ndi pa dzikolapansi ndi zanu; ufumu ndi wanu, Yehova; ndipomwakwezeka mutu wa pa zonse. Motero tsono,Mulungu wathu, tikuyamikani ndi kulemekezadzina lanu lokoma”. Masalimo 106:48; “Ndi anthuonse anene, Amen”. Chibvumbulutso 22:20; “Iyewakuchitira umboni izi anena indetu ndidza nsanga.Amen idzani Ambuye Yesu”.

MAFUNSO OBWEREZA:KUDZIWA MAYANKHO A MAFUNSO ONSEWA (107) KUTHANDIZA KUTI MOYOWANU WA UZIMU UKHALE WOZAMA NDI WOKHAZIDKIKA. PAJA MAU AKUTIANTHU ANGA AKUONONGEKA CHIFUKWA CHOSADZIWA. INU KHALANI ODZIWAKUTI MUSAONONGEKE!

1. Cholinga chenicheni chimene munthu ayenera kuchita kwa Mulungu ndi chiyani?2. Kodi ndi lamulo liti lomwe Mulungu wapereka lotitsogolera ife m’mwene

tingamlemekezere ndi kukondwerera mwa Iye?3. Kodi mawu a Mulungu kwenikweni amaphunzitsa chiyani?4. Kodi Mulungu ndi ndani?5. Kodi ilipo Milungu inanso?6. Kodi mu Umulungu muli anthu angati?7. Kodi malamulo a Mulungu ndi otani?8. Nanga Mulungu akukwaniritsa bwanji malamulo ake?9. Kodi ntchito ya chilengedwe ndi yotani?

10. Kodi munthu analengedwa bwanji?11. Kodi ntchito za Mulungu muchisamaliro chake ndi zotani?12. Kodi ndi chisamaliro chapadera chotani chimene Mulungu anaonetsera kwa munthu

m’munda umene analengedwera?13. Kodi makolo anthu oyamba anapitilira kukhalabe m’mene adalengedwera?14. Kodi tchimo ndi chiyani?

21

Page 22: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

15. Kodi ndi tchimo lanji limene linapangitsa makolo athu oyamba kugwa kuchokeram’manja mwa Mulungu?

16. Kodi mtundu wonse wa anthu unachimwanso pamene Adamu anachimwakoyamba?

17. Nanga kugwa kwa Adamu kunabweretsa chiyani ku mtundu wa anthu?18. Kodi tchimo limene linafikira munthu limapezeka mu chiyani?19. Kodi ndi masautso otani amene anabwera kwa munthu chifukwa cha uchimo?20. Kodi Mulungu analekelera mtundu wa anthu kuti uwonongeke m’machimo ndi

m’masautso awo?21. Kodi Mpulumutsi wa anthu osankhidwa a Mulungu ndi ndani?22. Kodi Khristu pokhala mwana wa Mulungu anakhala bwanji munthu?23. Kodi ndi maudindo ati amene Khristu ali nawo monga mombolo wathu?24. Kodi Khristu akugwira bwanji ntchito yake ya Uneneri?25. Kodi Khristu amagwira bwanji ntchito yake ya unsembe?26. Nanga Khristu anakwaniritsa bwanji udindo wake monga mfumu?27. Kodi kudzichepetsa kwa Khristu kunali kotani?28. Kodi kupambana kwa Yesu kunali kotani?29. Kodi timatenga nawo gawo bwanji ku chiwombolo chimene Khristu

anatibweretsera?30. Kodi Mzimu Woyera amatibweretsera bwanji chiwombolo cha Khristu?31. Kodi maitanidwe enieni ndi chiyani?32. Kodi pali phindu lanji limene oitanidwa amapeza mmoyo uno?33. Kodi kulungamitsidwa ndi chiyani?34. Kodi kukhala mwana wa Mulungu kukuthanthauza chiyani?35. Kodi chiyeretso ndi chiyani?36. Kodi ndi phindu lanji ku moyo uno limene limabwera chifukwa cha kulungamitsidwa,

kukhala mwana wa Mulungu, ndi kuyeretsedwa?37. Kodi ndi phindu lanji limene okhulupirira amalandira kuchokera kwa Khristu

akamwarira?38. Kodi ndi phindu lanji limene okhulupirira adzalandira pa tsiku lamdzukiro?39. Kodi udindo wa munthu kwa Mulungu ndi wotani?40. Kodi poyamba Mulungu anaulula chiyani kwa munthu palamulo la kumvera Iye?41. Kodi chilamulo tingachimvetse kuchokera ku chiyani?42. Kodi malamulo khumi amangidwa pa chiyani?43. Kodi mau otsogolera ku malamulo khumi ndi otani?44. Kodi mawu otsogolera ku Malamulo khumi akutiphunzitsa chiyani?45. Kodi lamulo loyamba ndi lotani?46. Kodi mulamulo loyambali akufuna chiyani?47. Kodi chimene chikuletsedwa mu lamulo loyamba ndi chiyani?48. Kodi makamaka tikuphunzira chiyani mulamulo ili loyamba mu mawu oti “Koma Inde

Ndekha”?49. Kodi lamulo lachiwiri ndi liti?50. Kodi mulamulo lachiwiri chikufunika ndi chiyani?51. Kodi mulamulo lachiwiri chimene chili kuletsedwa ndi chiyani?

22

Page 23: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

52. Kodi ndi mfundo zotani zimene zikupezeka mu lamulo lachiwiri?53. Kodi lamulo lachitatu ndi lotani?54. Kodi chikufunika ndi chiyani mu lamulo lachitatu?55. Kodi chikuletsedwa ndi chiyani mu lamulo lachitatu?56. Kodi ndi mfundo yotani imene ikupezeka mulamulo lachitatu?57. Kodi lamulo lachinayi ndi lotani?58. Kodi chifunika ndi chiyani mulamulo lachinayi?59. Kodi ndi tsiku liti mwa masiku asanu ndi awiri limene Mulungu anapatula kuti likhale

la Sabata?60. Nanga tsiku la Sabata liyenera kuyeretsedwa bwanji?61. Kodi chikuletsedwa ndi chiyani mu lamulo lachinayi?62. Kodi ndi mfundo zotani zimene zikupezeka mu lamulo lachinayili?63. Kodi lamulo lachisanu ndi liti?64. Kodi chikufunikira ndi chiyani mulamulo lachisanu?65. Nanga chikuletsedwa ndi chiyani mulamulo lachisanu?66. Kodi mulamulo limeneli tikupezamo mfundo yotani?67. Kodi lamulo lachisanu ndi chimodzi ndi liti?68. Kodi chikufunika ndi chiyani mu lamulo lachisanu ndi chimodzi?69. Kodi chikuletsedwa ndi chiyani mulamulo lachisanu ndi chimodzi?70. Kodi lamulo lachisanu ndi chiwiri ndi liti?71. Kodi chikufunikira ndi chiyani mulamulo lachisanu ndi chiwiri?72. Kodi chikuletsedwa ndi chiyani mu lamulo lachisanu ndi chiwiri?73. Kodi lamulo lachisanu ndi chitatu ndi liti?74. Kodi chikufunika ndi chiyani mu lamulo lachisanu ndi chitatu?75. Kodi chikuletsedwa ndi chiyani mulamulo lachisanu ndi chitatu?76. Kodi lamulo lachisanu ndi chinayi ndi liti?77. Kodi chikufunikira ndi chiyani mulamulo lachisanu ndi chinayi?78. Kodi chikuletsedwa ndi chiyani mulamulo lachisanu ndichinayi?79. Kodi lamulo lakhumi ndi liti?80. Kodi chikufunikira ndi chiyani mulamulo la khumi?81. Kodi chikuletsedwa ndi chiyani mulamulo la khumi?82. Kodi pali munthu aliyense amene angasunge mwangwiro malamulo a Mulungu?83. Kodi machimo ophwanya malamulo a Mulungu ndi ofanana kuopsya kwawo?84. Kodi tchimo lirilonse limayenera chiyani?85. Kodi Mulungu akufuna tichite chiyani kuti tipewe mkwiyo ndi temberero malingana

ndi tchimo lathu?86. Kodi chikhulupiriro mwa Yesu Khristu ndi chiyani?87. Kodi moyo wakulapa ndi chiyani?88. Kodi ndi njira ziti zime Khristu amationetsera ife ubwino wa chiombolo?89. Kodi Mau amapandigwa bwanji kukhala ndi mphamvu yopulumutsa?90. Nanga mawu angawerengedwe ndi kumveka bwanji kuti akhale ndi mphamvu

yopulumutsa?91. Kodi masakaramenti amakhala bwanji njira yachipulumutso?92. Kodi Sakaramenti ndi chiyani?

23

Page 24: CHIKHULUPIRIRO CHA AKHRISTU...osiyanasiyana ndi atsogoleri ena amene anasonkhana pa malo otchedwa Westminster, omwe ali mu Mzinda uja wotchuka wa London ku Magalande. Abusawatu amakonza

93. Kodi masakaramenti a Chipangano Chatsopano ndi ati?94. Kodi ubatizo ndi chiyani?95. Kodi ubatizo ungaperekedwe kwa yani?96. Kodi mgonero wa Ambuye ndi chiyani?97. Kodi chikufunikandi chiyani kwa iwo oyenera kulandira mgonero wa Ambuye?98. Kodi pemphero ndi chiyani?99. Kodi ndi lamulo lotani limene Mulungu wapereka lotitsogolera ku pemphero?

100. Kodi mau oyambirira pa pemphero la Ambuye amatiphunzitsa ife chiyani?101. Kodi timapempherera chiyani mugawo loyamba?102. Kodi timapempherera chiyani mu chigawo chachiwiri?103. Kodi timapempherera chiyani mu chigawo chachitatu?104. Kodi timapempherera chiyani mu chigawo chachinayi?105. Kodi timapempherera chiyani muchigawo chachisanu?106. Kodi timapempherera chiyani muchigawo chachisanu ndi chimodzi?107. Kodi kutsiriza kwa pemphero la Ambuye kumatiphunzitsa ife chiyani?

AMBUYE APITIRIZE KUDALITSA EVANGELICAL PRESBYTERIAN CHURCH (EPC)KUTI MAMEMBALA AKE ONSE ONSE AKHALE OCHITA MAU ANU MPAKAKUBWERA KWANU KWA CHIWIRI. ZIKOMO CHIFUKWA CHA MPINGO WATHUUMENENE UKUTSATIRA MAU ANU.

24